LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • km 1/14 tsa. 1
  • Ndandanda ya Mlungu wa January 13

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Ndandanda ya Mlungu wa January 13
  • Utimiki Wathu wa Ufumu—2014
  • Tumitu
  • MLUNGU WA JANUARY 13
Utimiki Wathu wa Ufumu—2014
km 1/14 tsa. 1

Ndandanda ya Mlungu wa January 13

MLUNGU WA JANUARY 13

Nyimbo 131 ndi Pemphelo

□ Phunzilo la Baibo la Mpingo:

jr mutu 3 ndime 1 mpaka 6 (Mph. 30)

□ Sukulu ya Ulaliki:

Kuŵelenga Baibo: Genesis 6–10 (Mph. 10)

Na. 1: Genesis 9:18–29 ndi 10:1-7 (Mph. 4 kapena zocepelapo)

Na. 2: Mmene Mungayankhile Ngati Wina Wanena Kuti, ‘Ngati Umakhulupilila Yesu, Palibe Vuto Ndi Chalichi Cimene Umakapemphelako’—rs tsa. 93 ndime 2 (Mph. 5)

Na. 3: Kodi Mkristu Angathetse Bwanji Cizoloŵezi Coseŵeletsa Malisece?—lv tsa. 218-219 (Mph. 5)

□ Msonkhano wa Nchito:

Nyimbo 69

Mph. 10: Kufunika Kobweleza Mfundo mu Utumiki Wakumunda. Nkhani yocokela m’buku la Sukulu ya Utumiki, patsamba 206 ndi 207. Mwacidule citani citsanzo cimodzi kapena ziŵili pa mfundo za m’nkhaniyi.

Mph. 10: Amuna Otumikila Bwino. (1 Tim. 3:13) Funsani atumiki othandiza aŵili. Kodi ali ndi maudindo otani mumpingo? Nanga maudindo ao aphatikizapo ciani? N’cifukwa ciani anakalamila kukhala atumiki othandiza? N’cifukwa ciani amadzipeleka kutumikila mumpingo ndi kuthandiza akulu? Ngati pampingo wanu palibe atumiki othandiza, kambilanani nkhani yocokela m’buku la Gulu mutu 6, pa kamutu kakuti “nchito zao.”

Mph. 10: “Tengelani Citsanzo kwa Aneneli—Mika.” Mafunso ndi mayankho.

Nyimbo 35 ndi Pemphelo

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani