LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • km 1/14 tsa. 3
  • Ndandanda ya Mlungu wa January 27

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Ndandanda ya Mlungu wa January 27
  • Utimiki Wathu wa Ufumu—2014
  • Tumitu
  • MLUNGU WA JANUARY 27
Utimiki Wathu wa Ufumu—2014
km 1/14 tsa. 3

Ndandanda ya Mlungu wa January 27

MLUNGU WA JANUARY 27

Nyimbo 106 ndi pemphelo

□ Phunzilo la Baibo la Mpingo:

jr mutu 3 ndime 13 mpaka 19 (Mph. 30)

□ Sukulu ya Ulaliki:

Kuŵelenga Baibo: Genesis 17–20 (Mph. 10)

Na. 1: Genesis 17:18–26 ndi 18:1-8 (Mph. 4 kapena zocepelapo)

Na. 2: Yesu Sanapite Kumwamba Ndi Thupi Lanyama—rs tsa. 107 ndime 2 ndi tsa. 108 ndime 2 (Mph. 5)

Na. 3: Kodi Babulo Wamkulu N’ciani?—bh tsa. 219-220 (Mph. 5)

□ Msonkhano wa Nchito:

Nyimbo 121

Mph. 5: Kuyambitsa Phunzilo la Baibo pa Ciŵelu Coyamba. Nkhani. Fotokozani makonzedwe amene apangidwa pampingo olalikila pa Ciŵelu coyamba mu February, ndipo limbikitsani onse kutengako mbali. Citani citsanzo cacidule mwa kugwilitsila nchito ulaliki wacitsanzo uli patsamba 4.

Mph. 15: Kodi Zolinga Zanu Zauzimu N’zotani? Kukambitsilana kocokela m’buku la Gulu, tsamba  117, ndime 2, mpaka kumapeto. Funsani wofalitsa mmodzi kapena aŵili amene anakwanilitsa colinga cao ca utumiki wa nthawi zonse. Kodi analimbikitsidwa bwanji ndi anthu ena? Kodi anagonjetsa zopinga zotani? Nanga ndi madalitso otani amene apeza?

Mph. 10: “Kupelekela Munthu Magazini Kumathandiza Kuyambitsa Maphunzilo a Baibo.” Mafunso ndi mayankho. Pemphani omvela kuti afotokoze mmene anayambitsila phunzilo la Baibo kwa munthu amene anali kumpelekela magazini.

Nyimbo 103 ndi Pemphelo

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani