LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • km 4/14 tsa. 2
  • Ndandanda ya Mlungu wa April 21

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Ndandanda ya Mlungu wa April 21
  • Utimiki Wathu wa Ufumu—2014
  • Tumitu
  • MLUNGU WA APRIL 21
Utimiki Wathu wa Ufumu—2014
km 4/14 tsa. 2

Ndandanda ya Mlungu wa April 21

MLUNGU WA APRIL 21

Nyimbo 132 ndi Pemphelo

Phunzilo la Baibulo la Mpingo:

jr mutu 7 ndime 7-13 (Mph. 30)

Sukulu ya Ulaliki:

Kuŵelenga Baibulo: Ekisodo 15-18 (Mph. 10)

Na. 1: Ekisodo 15:20 mpaka 16:5 (Mph. 4 kapena zocepelapo)

Na. 2: Akristu Safunikila Kusunga Sabata—rs tsa. 346 ¶2-3 (Mph. 5)

Na. 3: N’cifukwa Ciani Tiyenela Kuona Moyo Monga Mphatso Yamtengo Wapatali Yocokela kwa Mulungu—bh-tsa. 125-127 ndime 3-5 ndi lv- tsa. 80 ndime 16 (Mph. 5)

Msonkhano wa Nchito:

Nyimbo 27

Mph. 10: Kodi Mwakonzekela Kulimbana Ndi Mayeselo Kusukulu? Nkhani yokambilana. Pemphani omvela kuti afotokoze ena mwa mavuto amene Akristu acinyamata amakumana nao kusukulu. Fotokozani mmene makolo angagwilitsilile nchito buku la Index, mabuku a Zimene Achinyamata Amafunsa, Webu saiti yathu, ndi zofalitsa zina, pa kulambila kwa pabanja kuti akonzekeletse ana ao kulimbana ndi mayeselo amene adzakumana nao ku sukulu. (1 Pet. 3:15) Sankhani nkhani imodzi kapena ziŵili, ndipo fotokozani mfundo zothandiza zimene zikupezeka m’zofalitsa zathu. Pemphani omvela kuti afotokoze zimene anacita kuti athe kulalikila kusukulu.

Mph. 20: Zosoŵa za pampingo.

Nyimbo 125 and Pemphelo

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani