LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • km 5/14 tsa. 1
  • Ndandanda ya Mlungu wa May 12

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Ndandanda ya Mlungu wa May 12
  • Utimiki Wathu wa Ufumu—2014
  • Tumitu
  • MLUNGU WA MAY 12
Utimiki Wathu wa Ufumu—2014
km 5/14 tsa. 1

Ndandanda ya Mlungu wa May 12

MLUNGU WA MAY 12

Nyimbo 49 ndi Pemphelo

Phunzilo la Baibulo la Mpingo:

jr mutu 8 ndime 8-13 (Mph. 30)

Sukulu ya Ulaliki:

Kuŵelenga Baibulo: Ekisodo 27-29 (Mph. 10)

Na. 1: Ekisodo 29:19-30 (Mph. 4 kapena zocepelapo)

Na. 2: Yesu Sanagawe Cilamulo ca Mose Kukhala ndi Mbali ya “Mwambo” ndi ya “Makhalidwe Abwino”—rs tsa. 347 ndime 3 mpaka tsa. 348 ndime 1 (Mph. 5)

Na. 3: Kodi Tingatani Kuti Tisiye Kugwilizana ndi Mizimu Yoipa?—bh tsa. 103-104 ndime 14 mpaka 16 (Mph. 5)

Msonkhano wa Nchito:

Nyimbo 75

Mph. 15: Mitundu Yonse Idzakhamukila Kumeneko. (Yes. 2:2) Funsani ofalitsa aŵili, mmodzi akhale amene wakhala m’coonadi zaka zambili ndipo winayo akhale watsopano. N’ciani cinawakopa kuti ayambe kuphunzila coonadi? Kodi ndi mavuto otani amene anakumana nao ndipo anawathetsa bwanji? N’ciani cinawasangalatsa kwambili nthaŵi yoyamba imene anapezeka pamisonkhano yampingo? Kodi amakumbukila ciani nthawi yoyamba imene anapita mu ulaliki? Kodi ofalitsa ena mumpingo anawathandiza bwanji kuti apite patsogolo mwa kuuzimu?

Mph. 15: “Kuongolela Luso Lathu mu Ulaliki—Kukonzekela Mau Athu Oyamba.” Kukambilana. Citani citsanzo cacidule ca mbali ziŵili. Mbali yoyamba ioonetse wofalitsa akugwilitsila nchito mau oyamba osakonzekela bwino ndipo yaciŵili ioonetse mau oyamba okonzedwa bwino. Ngati nthawi ilola fotokozani mfundo zimene zingakhale zothandiza zocokela m’buku la Sukulu ya Utumiki, masamba 215 mpaka 219.

Nyimbo 117 ndi Pemphelo

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani