LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • km 7/14 tsa. 2
  • Ndandanda ya Mlungu wa July 21

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Ndandanda ya Mlungu wa July 21
  • Utimiki Wathu wa Ufumu—2014
  • Tumitu
  • MLUNGU WA JULY 21
Utimiki Wathu wa Ufumu—2014
km 7/14 tsa. 2

Ndandanda ya Mlungu wa July 21

MLUNGU WA JULY 21

Nyimbo 73 ndi Pemphelo

Phunzilo la Baibulo la Mpingo:

jr mutu 11 ndime 9 mpaka 14 (Mph. 30)

Sukulu ya Ulaliki:

Kuŵelenga Baibulo: Levitiko 25-27 (Mph. 10)

Na. 1: Levitiko 26:1-17 (Mph. 4 kapena zocepelapo)

Na. 2: Kodi Anthu Onse Pomalizila Pake Adzapulumutsidwa?—rs tsa. 95 ndime 1 (Mph. 5)

Na. 3: Mmene Malemba Amasiyanitsila Ngozi Yeniyeni Ndi Zinthu Zadala—lv tsa. 84 ndime 23-25 (Mph. 5)

Msonkhano wa Nchito:

Nyimbo 67

Mph. 10: Timapatsidwa Ulemu Cifukwa ca Khalidwe Lathu Labwino ndi Kusatengako Mbali M’zandale. Nkhani yokambilana yocokela mu Buku Lapacaka la 2014, masamba 120 ndi 149. Pemphani omvela kuti anene zimene aphunzilapo.

Mph. 10: Kodi Mudzacitako Upainiya Wothandiza m’Mwezi wa August? Nkhani. Funsani mafunso ofalitsa aŵili kapena atatu amene aganiza zocita upainiya m’mwezi wa August ngakhale kuti ndi odwala kapena ndi otangwanika ndi zinthu zina. Kodi ndi zinthu ziti zimene aona kuti afunika kusintha n’colinga cakuti akacite upainiya? Pemphani woyang’anila nchito kuti anene makonzedwe a utumiki wa kumunda amene mpingo wapanga m’mwezi wa August.

Mph. 10: “Kodi Yehova Amandiona Bwanji?” Mafunso ndi mayankho.

Nyimbo 65 ndi Pemphelo

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani