LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • km 8/14 tsa. 2
  • Ndandanda ya Mlungu wa August 18

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Ndandanda ya Mlungu wa August 18
  • Utimiki Wathu wa Ufumu—2014
  • Tumitu
  • MLUNGU WA AUGUST 18
Utimiki Wathu wa Ufumu—2014
km 8/14 tsa. 2

Ndandanda ya Mlungu wa August 18

MLUNGU WA AUGUST 18

Nyimbo 78 ndi Pemphelo

Phunzilo la Baibulo la Mpingo:

jr mutu 12 ndime 14 mpaka 19, bokosi pa tsa. 148 (Mph. 30)

Msonkhano wa Nchito:

Kuŵelenga Baibulo: Numeri 10-13 (Mph. 10)

Na. 1: Numeri 10:1-16 (Mph. 4 kapena zocepelapo)

Na. 2: Cifukwa Cake Cikhulupililo Ciyenela Kukhala ndi Nchito—rs tsa. 97 ndime 1-4 (Mph. 5)

Na. 3: Dina ndi Citsanzo Coticenjeza—lv tsa. 102-103 ndime 13-15 (Mph. 5)

Msonkhano wa Nchito:

Nyimbo 74

Mph. 15: “Zaka 100 Zolengeza Ufumu”—Mbali 1. (Ndime 1-3) Nkhani yokambilana yocokela pa ndime zitatu zoyambilila ndiponso mu Nsanja ya Mlonda ya January 1, 2014 masamba 13-15 ndime 7-11. Mukafunsa funso la m’ndime 3, funsani ofalitsa aŵili amene akhala Mboni kwa nthaŵi yaitali. Apempheni kuti afotokoze zocitika za mu ulaliki nthawi yoyamba imene anakhala ofalitsa.

Mph. 15: “Zaka 100 Zolengeza Ufumu”—Mbali 2. (Ndime 4-6) Mafunso ndi mayankho. Pokambilana ndime 5 ndi 6, funsani apainiya aŵili kuti afotokoze zimene zawathandiza kukwanitsa kucita utumiki wa nthawi zonse.

Nyimbo 103 ndi Pemphelo

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani