LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • km 9/14 tsa. 4
  • Zocitika Zokhudza Ulaliki

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Zocitika Zokhudza Ulaliki
  • Utimiki Wathu wa Ufumu—2014
Utimiki Wathu wa Ufumu—2014
km 9/14 tsa. 4

Zocitika Zokhudza Ulaliki

Ndife osangalala kuona kuti ofalitsa ndiponso apainiya akupeleka lipoti la kuculuka kwa tumapepala twauthenga ndi mabulosha amene agaŵila mu ulaliki mwezi uliwonse. M’mwezi wa March 2014, tinali ndi ciŵelengelo capamwamba cokwana 754,535 ca tumapepala twauthenga ndi mabulosha amene anafalitsidwa. Tikuyamikila kwambili nchito imene munagwila! Cifukwa ca khama lanu, tinalinso ndi ciŵelengelo capamwamba ca maulendo obwelelako okwana 1,787,395 amene anapangidwa kwa anthu acidwi. Ndife otsimikiza kuti “Mwini zokolola” adzadalitsa khama lanu lobzala ndi kuthilila mbeu za coonadi kwa anthu acidwi, ndipo adzapitiliza ‘kukulitsa’ mbeuzo.—Mat. 9:38; 1 Akor. 3:6.

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani