LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • km 11/14 tsa. 1
  • Ndandanda ya Mlungu wa November 10

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Ndandanda ya Mlungu wa November 10
  • Utimiki Wathu wa Ufumu—2014
  • Tumitu
  • MLUNGU WA NOVEMBER 10
Utimiki Wathu wa Ufumu—2014
km 11/14 tsa. 1

Ndandanda ya Mlungu wa November 10

MLUNGU WA NOVEMBER 10

Nyimbo 99 ndi Pemphelo

Phunzilo la Baibulo la Mpingo:

jr mutu 15 ndime 13 mpaka 20 (Mph. 30)

Sukulu ya Ulaliki:

Kuŵelenga Baibulo: Deuteronomo 19-22 (Mph. 10)

Na. 1: Deuteronomo 22:20-30 (Mph. 4 kapena zocepelapo)

Na. 2: Mmene Ucimo Umakhudzila Ubwenzi Wathu ndi Mulungu—rs tsa. 361 ndime 1–4(Mph. 5)

Na. 3: Kodi Baibulo Limati Ciani pa Nkhani Yopatukana?—lv tsa. 220 ndime 2-tsa. 221 (Mph. 5)

Msonkhano wa Nchito:

Nyimbo 12

Mph. 10: Funsani Mafunso Woyang’anila Nchito. Kodi kusamalila nchito yanu kumaphatikizapo ciani? Ndi zinthu ziti zimene mumayesetsa kucita mukamacezela kagulu ka ulaliki? Kodi amene ali m’kagulu angacite ciani kuti apindule kwambili ndi kucezetsa kwanu? Mumathandiza bwanji ofalitsa amene akufikilani kuti muwathandize pa mbali inayake ya ulaliki?

Mph. 20: “Kunola Luso Lathu mu Ulaliki—Kuonetsa Anthu Cidwi.” Kukambilana. Pambuyo pa kukambilana nkhaniyi, citani citsanzo ca mbali ziŵili. Mbali yoyamba, wofalitsa asaonetse cidwi kwa munthu amene akumugaŵila cofalitsa ca mwezi umenewo. Koma mbali yaciŵili, wofalitsa aonetse cidwi kwa munthu amene akumugaŵila cofalitsa.

Nyimbo 84 ndi Pemphelo

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani