LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • km 4/15 tsa. 1
  • Ndandanda ya Mlungu wa April 13

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Ndandanda ya Mlungu wa April 13
  • Utimiki Wathu wa Ufumu—2015
  • Tumitu
  • MLUNGU WA APRIL 13
Utimiki Wathu wa Ufumu—2015
km 4/15 tsa. 1

Ndandanda ya Mlungu wa April 13

MLUNGU WA APRIL 13

Nyimbo 134 ndi Pemphelo

Phunzilo la Baibulo la Mpingo:

cl mutu 8 ndime 1-8 (Mph. 30)

Sukulu ya Ulaliki:

Kuŵelenga Baibulo: 1 Samueli 19-22 (Mph. 8)

Na. 1: 1 Samueli 21:10–22:4 (Mph. 3 kapena zocepelapo)

Na. 2: Baranaba—Mutu: Khalani Okoma Mtima—w14 6/1 tsa. 24 ndime 13 (Mph. 5)

Na. 3: N’cifukwa Ciani Anthu Amavutika?—igw-CIN tsa 15 ndime 1-4 (Mph. 5)

Msonkhano wa Nchito:

Lemba la Mwezi: Yendani monga anthu anzelu mwa ‘kugwilitsila nchito bwino nthawi yanu.’—Aef. 5:15, 16.

Nyimbo 115

Mph. 10: Yendani Monga Anthu Anzelu mwa “Kugwilitsila Nchito Bwino Nthawi yanu.” Nkhani yofotokoza lemba la mwezi.—Aef. 5:15, 16; onani Nsanja ya Olonda ya, May 15, 2012, mas. 19-20, ndime 11-14.

Mph. 20: “Muzigwilitsa Nchito Bwino Nthawi Yanu mu Ulaliki.” Kukambilana.

Nyimbo 98 ndi Pemphelo

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani