LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • km 8/15 tsa. 2
  • Ndandanda ya Mlungu wa August 17

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Ndandanda ya Mlungu wa August 17
  • Utimiki Wathu wa Ufumu—2015
  • Tumitu
  • MLUNGU WA AUGUST 17
Utimiki Wathu wa Ufumu—2015
km 8/15 tsa. 2

Ndandanda ya Mlungu wa August 17

MLUNGU WA AUGUST 17

Nyimbo 5 ndi Pemphelo

Phunzilo la Baibulo la Mpingo:

cl mutu 14 ndime 1-9 (Mph. 30)

Sukulu ya Ulaliki:

Kuŵelenga Baibulo: 2 Mafumu 1-4 (Mph. 8)

Na. 1: 2 Mafumu 1:11-18 (Mph. 3 kapena zocepelapo)

Na. 2: Dina—Mutu: Kugwilizana ndi Anthu Oipa Kumabweletsa Mavuto—w10 6/15 tsa. 8-9 ndime 13-15 (Mph. 5)

Na. 3: Zimene Tiyenela Kucita Kuti Tiyandikile Mulungu—igw-CIN tsa. 28 ndime 5–tsa. 29 ndime 1-3 (Mph. 5)

Msonkhano wa Nchito:

Lemba la Mwezi: “Koma ine ndi a m’nyumba yanga, tizitumikila Yehova.”—Yoswa 24:15.

Nyimbo 52

Mph. 15: “Makolo—Wetani Ana Anu.” Nkhani yokambilana yocokela mu Nsanja ya Mlonda ya September 15, 2014 masamba 17 mpaka 21. Kambani mau oyamba acidule, kenako kambilanani mfundo zikuluzikulu za m’nkhaniyi zimene makolo angagwilitsile nchito.

Mph 15: Kodi Anagwila Bwanji Dzanja Lanu? (Yes 41:13)Funsani mafunso wofalitsa mmodzi kapena aŵili amene atumikila mokhulupilika kwa zaka zambili, kuti afotokoze mmene Yehova wawathandizila kulimbana ndi mavuto pomutumikila.

Nyimbo 88 ndi Pemphelo

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani