LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • km 11/15 tsa. 2
  • Ndandanda ya Mlungu wa November 16

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Ndandanda ya Mlungu wa November 16
  • Utimiki Wathu wa Ufumu—2015
  • Tumitu
  • MLUNGU WA NOVEMBER 16
Utimiki Wathu wa Ufumu—2015
km 11/15 tsa. 2

Ndandanda ya Mlungu wa November 16

MLUNGU WA NOVEMBER 16

Nyimbo 17 ndi Pemphelo

Phunzilo la Baibulo la Mpingo:

ia mutu 2 ndime 13-23, ndi kubwelelamo pa tsa. 24 (Mph. 30)

Sukulu ya Ulaliki:

Kuŵelenga Baibulo: 1 Mbiri 26-29 (Mph. 8)

Na. 1: 1 Mbiri 29:20-30 (Mph. 3 kapena zocepelapo)

Na. 2: Kodi “Nsembe Yophimba Macimo” Imatanthauza Ciani? (Mph. 5)

Na. 3: Elizabeti—Mutu: Muziopa Mulungu ndi Kupewa Zoipa—w11 1/15 tsa. 13-14 ndime 5-7 (Mph. 5)

Msonkhano wa Nchito:

Lemba la Mwezi: “Ineyo ndinabzala, Apolo anathilila, koma Mulungu ndiye anakulitsa.”—1 Akor. 3:6.

Nyimbo 35

Mph.10: Pitilizani Kukulitsa Cidwi ca Anthu Amene Mumalalikila. (1 Akor. 3:6-8) Funsani mafunso mpainiya wa nthawi zonse ndi wofalitsa. Kodi anapanga bwanji ndandanda yocita maulendo obwelelako? Nanga amakonzekela bwanji? Kodi amacita bwanji akapeza kuti munthu amene analalikila pa ulendo woyamba sali panyumba? Nanga ndi madalitso otani amene io apeza?

Mph.20: “Mmene Tingagwilitsile Nchito Zinthu Zongomvetsela za pa jw.org.” Mafunso ndi mayankho. Fotokozani mmene ofalitsa angapezele zinthu zongomvetsela za pa jw.org. Lizani nkhani imodzi monga citsanzo ku gulu. Ndiyeno, citani citsanzo ca cocitika cimene cili kumapeto kwa nkhani yakuti “Gwilitsilani Nchito Webusaiti Yathu mu Ulaliki—‘Kuyankha Mafunso a m’Baibulo,’” mu Utumiki Wathu wa Ufumu wa November 2014.

Nyimbo 108 ndi Pemphelo

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani