LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • km 11/15 tsa. 3
  • Ndandanda ya Mlungu wa November 23

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Ndandanda ya Mlungu wa November 23
  • Utimiki Wathu wa Ufumu—2015
  • Tumitu
  • MLUNGU WA NOVEMBER 23
Utimiki Wathu wa Ufumu—2015
km 11/15 tsa. 3

Ndandanda ya Mlungu wa November 23

MLUNGU WA NOVEMBER 23

Nyimbo 26 ndi Pemphelo

Phunzilo la Baibulo la Mpingo:

ia mutu 3 ndime 1-13, ndi bokosi pa tsa. 29 (Mph. 30)

Sukulu ya Ulaliki:

Kuŵelenga Baibulo: 2 Mbiri 1-5 (Mph. 8)

Na. 1: 2 Mbiri 3:14–4:6 (Mph. 3 kapena zocepelapo)

Na. 2: Inoki—Mutu: Muziyenda Ndi Mulungu—w11 11/15 tsa.16 ndime 2 (Mph. 5)

Na. 3: Kodi Pali Mitundu Ingati ya Ubatizo? (Mph. 5)

Msonkhano wa Nchito:

Lemba la Mwezi: “Ineyo ndinabzala, Apolo anathilila, koma Mulungu ndiye anakulitsa.”—1 Akor. 3:6.

Nyimbo 47

Mph.10: “Kukonzekela n’Kofunika Kuti Tiziphunzitsa Mwaluso.” Nkhani.

Mph.10: Kukhala ndi Khalidwe Labwino Kumatithandiza Kubzala Mbeu za Coonadi. Kukambilana kocokela m’Buku Lapacaka la 2015 tsamba 49 ndime 3 mpaka tsamba 51 ndime 3, ndi tsamba 140 ndime 3 mpaka tsamba 141 ndime 3. Pemphani omvela kuti akambe zimene aphunzilapo.

Mph.10: “Seŵenzetsani Zinthu Zopezeka m’Buku la Zimene Baibo Imaphunzitsa Mogwila Mtima.” Kukambilana. Mucitenso citsanzo cacidule.

Nyimbo 123 ndi Pemphelo

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani