LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • km 11/15 tsa. 4
  • Ndandanda ya Mlungu wa November 30

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Ndandanda ya Mlungu wa November 30
  • Utimiki Wathu wa Ufumu—2015
  • Tumitu
  • MLUNGU WA NOVEMBER 30
Utimiki Wathu wa Ufumu—2015
km 11/15 tsa. 4

Ndandanda ya Mlungu wa November 30

MLUNGU WA NOVEMBER 30

Nyimbo 94 ndi Pemphelo

Phunzilo la Baibulo la Mpingo:

ia mutu 3 ndime 14-21, ndi bokosi pa tsa. 30, ndiponso kubwelelamo pa tsa. 32 (Mph. 30)

Sukulu ya Ulaliki:

Kuŵelenga Baibulo: 2 Mbiri 6-9 (Mph. 8)

Na. 1: 2 Mbiri 6:22-27 (Mph. 3 kapena zocepelapo)

Na. 2: Kodi Kupulupudza Kwamwano N’koipa Motani? (Mph. 5)

Na. 3: Epafura—Mutu: Muzitumikila Abale Anu ndi Kuwapemphelela—w13 11/15 tsa. 6 ndime 15 (Mph. 5)

Msonkhano wa Nchito:

Lemba la Mwezi: “Ineyo ndinabzala, Apolo anathilila, koma Mulungu ndiye anakulitsa.”—1 Akor. 3:6.

Nyimbo 58

Mph.10: Kugaŵila magazini mu December. Kukambilana. Yambani mwa kucita zitsanzo ziŵili poseŵenzetsa maulaliki acitsanzo patsamba lino. Ndiyeno, kambilanani maulaliki onse acitsanzo.

Mph.10: Zosoŵa za Pampingo.

Mph.10: Tinacita Zotani? Kukambilana. Pemphani omvela kuti akambe mapindu amene apeza pogwilitsila nchito mfundo za m’nkhani yakuti, “Kunola Luso Lathu mu Ulaliki—Kugaŵila Buku la Zimene Baibo Imaphunzitsa.” Ndiyeno, apemphani kuti afotokoze zocitika zosangalatsa za mu ulaliki.

Nyimbo 141 ndi Pemphelo

Cikumbutso: Lizani nyimbo yatsopanoyo kamodzi, kenako mpingo uimbile pamodzi nyimboyo.

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani