LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • km 12/15 tsa. 4
  • Ndandanda ya Mlungu wa December 28

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Ndandanda ya Mlungu wa December 28
  • Utimiki Wathu wa Ufumu—2015
  • Tumitu
  • MLUNGU WA DECEMBER 28
Utimiki Wathu wa Ufumu—2015
km 12/15 tsa. 4

Ndandanda ya Mlungu wa December 28

MLUNGU WA DECEMBER 28

Nyimbo 79 ndi Pemphelo

Phunzilo la Baibulo la Mpingo:

ia mutu 5 ndime 14-26, ndi kubwelelamo pa tsa. 50 (Mph. 30)

Sukulu ya Ulaliki:

Kuŵelenga Baibulo: 2 Mbiri 25-28 (Mph. 8)

Kubweleza za m’Sukulu ya Ulaliki (Mph. 20)

Msonkhano wa Nchito:

Lemba la Mwezi: “Tiyenela kukumana ndi masautso ambili kuti tikaloŵe mu Ufumu wa Mulungu.”—Machitidwe 14:22.

Nyimbo 122

Mph.15: Muzipemphelela Abale Anu. Kukambilana. Yambani ndi kuŵelenga Machitidwe 12:1-11. Ndiyeno, kambilanani mfundo zofunika za m’buku la Kucitira Umboni masamba 77-80, ndime 5-12. Pambuyo pake, ngati mumapita pa Intaneti, chulani nkhani zaposacedwapa zopezeka pa jw.org. Pitani polemba kuti “Malo a Nkhani” (Newsroom). Limbikitsani onse kuti azipemphelela abale amene akukumana ndi mayeselo osiyanasiyana padziko lonse. Ndipo ngati n’kotheka, azichula maina a abalewo m’mapemphelo ao.—2 Akor. 1:11; 1 Tim. 2:1, 2.

Mph.15: Zosoŵa za Pampingo.

Nyimbo 124 ndi Pemphelo

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani