LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb16 August tsa. 3
  • Khalanibe m’Malo Otetezeka a Wam’mwambamwamba

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Khalanibe m’Malo Otetezeka a Wam’mwambamwamba
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Msonkhano (2016)
  • Nkhani Zofanana
  • Zamkati
    Galamuka!—2018
  • Cisinsi Cimene Ndife Okondwela Kudziŵa
    Phunzitsani Ana Anu
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Msonkhano (2016)
mwb16 August tsa. 3

CUMA COPEZEKA M’MAU A MULUNGU | MASALIMO 87–91

Khalanibe m’Malo Otetezeka a Wam’mwambamwamba

“Malo Otetezeka” a Yehova amatithandiza kukhala otetezeka mwauzimu

91:1, 2, 9-14

  • Kuti tikhale m’malo otetezeka a Yehova, tifunika kudzipeleka ndi kubatizika

  • Amene sakhulupilila Mulungu, sawadziŵa malo otetezeka amenewa

  • Amene ali m’malo otetezeka a Yehova, salola kuti munthu wina kapena cinthu cina ciwalepheletse kukhulupilila Mulungu kapena kumukonda

“Wosaka mbalame” amachela misampha kuti atigwile

91:3

  • Mbalame n’zocenjela, ndipo n’zovuta kuzigwila

  • Wosaka mbalame amaona mmene mbalame zimacitila zinthu, ndipo amapeza njila yozigwilila

  • Satana, amene ndi “wosaka mbalame,” amaona zimene atumiki a Yehova amacita, ndipo amachela misampha kuti awaononge mwauzimu

Mbalame ikuyang’ana msampha ndipo wosaka mbalame wabisala capafupi

Misampha inayi yowononga imene Satana amaseŵenzetsa:

  • Mkhiristu wa m’nthawi ya atumwi athaŵa anthu ozunza Akhiristu

    Kuwopa Anthu

  • Muulu wa ndalama

    Kukonda Cuma

  • Banja la m’nthawi ya atumwi lituluka m’bwalo la maseŵela la Aroma

    Zosangulutsa Zoipa

  • Anthu aŵili a m’nthawi ya atumwi akangana

    Mikangano

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani