LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb19 May tsa. 4
  • May 20-26

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • May 20-26
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2019
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2019
mwb19 May tsa. 4

May 20-26

2 AKORINTO 11-13

  • Nyimbo 3 na Pemphelo

  • Mawu Oyamba (3 min. olo kucepelapo)

CUMA COPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

  • “‘Munga M’thupi’ la Paulo”: (10 min.)

    • 2 Akor. 12:7—Paulo analimbana na vuto limene linali ngati munga wopweteka (w08 6/15 3-4)

    • 2 Akor. 12:8, 9—Yehova anasankha kusayankha pembedzelo la Paulo lakuti amucotsele vutolo (w06 12/15 24 ¶17-18)

    • 2 Akor. 12:10—Paulo anakwanilitsa utumiki wake mwa kudalila mzimu woyela wa Mulungu (w18.01 9 ¶8-9)

  • Kufufuza Cuma ca Kuuzimu: (8 min.)

    • 2 Akor. 12:2-4—Kodi “kumwamba kwacitatu” komanso “paradaiso” ziyenela kuti zitanthauza ciani? (w18.12 8 ¶10-12)

    • 2 Akor. 13:12—Kodi mawu akuti “kupsompsonana kwaubale” amanena za ciani? (it-2 177)

    • Kodi imwe pacanu, kuŵelenga Baibo kwa wiki ino kwakuphunzitsani ciani za Yehova?

    • Ni cuma ca kuuzimu cina citi cimene mwapeza pa kuŵelenga Baibo kwa wiki ino?

  • Kuŵelenga Baibo: (4 min. olo kucepelapo) 2 Akor. 11:1-15 (th phunzilo 5)

CITANI KHAMA PA ULALIKI

  • Vidiyo ya Ulendo Wobwelelako Woyamba: (5 min.) Tambitsani na kukambilana vidiyoyi.

  • Ulendo Wobwelelako Woyamba: (3 min. olo kucepelapo ) Seŵenzetsani makambilano acitsanzo. (th phunzilo 2)

  • Ulendo Wobwelelako Woyamba: (4 min. olo kucepelapo) Yambani na makambilano acitsanzo, ndiyeno gaŵilani buku la Zimene Baibulo Ingatiphunzitse. (th phunzilo 4)

UMOYO WATHU WACIKHRISTU

  • Nyimbo 38

  • “Mungapambane Ngakhale Kuti Muli na ‘Munga M’thupi’!”: (15 min.) Kukambilana. Tambitsani vidiyo yakuti “Maso a anthu akhungu adzatseguka”. Dziŵitsani omvetsela kuti mabuku a akhungu kapena kuti a anthu osaona apezeka mu zitundu 47, m’kalembedwe ka akhungu komanso m’mitundu ina. Ofalitsa afunika kuuza mtumiki wa mabuku kuti aitanitse mabukuwo. Limbikitsani omvetsela onse kuti azikhala chelu komanso okonzeka kuthandiza aliyense amene ni wakhungu mumpingo kapena m’gawo.

  • Phunzilo la Baibo la Mpingo: (30 min.) jy mutu 67

  • Kubwelelamo na Kuchulako za Wiki Yotsatila (3 min.)

  • Nyimbo 78 na Pemphelo

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani