LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb19 May tsa. 4
  • “Munga M’thupi” la Paulo

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • “Munga M’thupi” la Paulo
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2019
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2019
mwb19 May tsa. 4

CUMA COPEZEKA M’MAWU A MULUNGU | 2 AKORINTO 11-13

“Munga M’thupi” la Paulo

12:7-10

Nthawi zambili, Baibo imaseŵenzetsa liwu lakuti minga mlingalilo lophiphilitsa. Minga zingatanthauze anthu ovutitsa ena kapena amene amavulaza ena. Zingatanthauzenso zinthu zimene zingabweletse mavuto. (Num. 33:55; Miy. 22:5; Ezek. 28:24) Paulo, polemba za “munga m’thupi,” mwina anali kutanthauza atumwi onyenga, kapenanso anthu ena amene anali kukayikila utumwi wake na nchito zake. Kodi malemba ali munsimu aonetsa zinthu zina ziti zimene mwina zinali “munga m’thupi” kwa Paulo?

  • Mtumwi Paulo akugwila ku mutu

    Mac. 23:1-5

  • Agal. 4:14, 15

  • Agal. 6:11

Nanga imwe, ‘munga wanu m’thupi’ n’ciani?

Ndipo mungadalile motani pa Yehova kuti akuthandizeni kuupilila?

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani