LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb20 July tsa. 4
  • July 20-26

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • July 20-26
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2020
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2020
mwb20 July tsa. 4

July 20-26

EKSODO 10-11

  • Nyimbo 65 na Pemphelo

  • Mawu Oyamba (1 min.)

CUMA COPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

  • “Mose na Aroni Anaonetsa Kulimba Mtima Kwambili”: (10 min.)

    • Eks 10:3-6—Molimba mtima Mose na Aroni analengeza mlili wa namba 8 kwa Farao (w09 7/15 20 ¶6)

    • Eks. 10:24-26—Mose na Aroni sanagonje pamene Farao anayesa kuwanyengelela kuti asalabadile zonse zimene Yehova anawalamula

    • Eks. 10:28; 11:4-8—Mopanda mantha Mose na Aroni analengeza mlili wa namba 10 (it-2 436 ¶4)

  • Kufufuza Cuma ca Kuuzimu: (10 min.)

    • Eks. 10:1, 2—Kodi makolo angaphunzile ciani pa mavesiwa? (w95 9/1 11 ¶11)

    • Eks. 11:7—Kodi Yehova anatanthauza ciani pamene anakamba kuti “galu sadzauwa aliyense wa ana a Isiraeli”? (it-1 783 ¶5)

    • Pa kuŵelenga Baibo kwa wiki ino, ni mfundo yopindulitsa iti imene munapeza yokhudza Yehova Mulungu, ulaliki, kapena mfundo ina iliyonse?

  • Kuŵelenga Baibo: (4 min. olo kucepelapo) Eks 10:1-15 (th phunzilo 10)

CITANI KHAMA PA ULALIKI

  • Vidiyo ya Ulendo Wobwelelako: (5 min.) Kukambilana. Tambitsani vidiyoyi, ndiyeno funsani mafunso otsatilawa: Kodi mwaphunzilapo ciani poona mmene wofalitsa wakambila na mwininyumba? Kodi wofalitsa akanacita ciani kuti agaŵile cofalitsa ca mu Thuboksi Yathu?

  • Ulendo Wobwelelako: (4 min. olo kucepelapo) Yambani na makambilano acitsanzo. Ndiyeno Itanilani mwininyumba ku misonkhano. (th phunzilo 8)

  • Ulendo Wobwelelako: (4 min. olo kucepelapo) Yambani na makambilano acitsanzo. Ndiyeno gaŵilani cofalitsa ca mu Thuboksi Yathu. (th phunzilo 12)

UMOYO WATHU WACIKHRISTU

  • Nyimbo 55

  • “Kodi Zolengedwa Zimatiphunzitsa Ciani za Kulimba Mtima?”: (15 min.) Kukambilana. Tambitsani vidiyo yakuti Tiphunzile Kulimba Mtima ku Zolengedwa.

  • Phunzilo la Baibo la Mpingo: (30 min.) jy mutu 124

  • Mawu Othela (3 min. olo kucepelapo)

  • Nyimbo 113 na Pemphelo

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani