LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb20 December tsa. 4
  • December 14-20

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • December 14-20
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2020
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2020
mwb20 December tsa. 4

December 14-20

LEVITIKO 12-13

  • Nyimbo 140 na Pemphelo

  • Mawu Oyamba (1 min.)

CUMA COPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

  • “Phunzilamponi Kanthu pa Malamulo Okhudza Nthenda ya Khate”: (10 min.)

    • Lev. 13:4, 5—Anthu odwala khate anali kuwaika kwaokha (wp18.1 7)

    • Lev. 13:45, 46—Anthu akhate anali kufunika kupewa kufalitsa matendawo kwa ena (wp16.4 9 ¶1)

    • Lev. 13:52, 57—Zinthu zimene pafalikila matendawa zinali kuwonongedwa (it-2 238 ¶3)

  • Kufufuza Cuma ca Kuuzimu: (10 min.)

    • Lev. 12:2, 5—N’cifukwa ciani mkazi anali kukhala “wodetsedwa” akabeleka mwana? (w04 5/15 23 ¶2)

    • Lev 12:3—Kodi mwina n’cifukwa ciani Yehova analamula kuti ana azidulidwa pa tsiku la 8? (wp18.1 7)

    • Pa kuŵelenga Baibo kwa wiki ino, ni mfundo yopindulitsa iti imene munapeza yokhudza Yehova, ulaliki, kapena mfundo ina iliyonse?

  • Kuŵelenga Baibo: (4 min. olo kucepelapo) Lev. 13:9-28 (th phunzilo 5)

CITANI KHAMA PA ULALIKI

  • Vidiyo ya Ulendo Wobwelelako: (4 min.) Kukambilana. Tambitsani vidiyo imeneyi. Ndiyeno funsani omvetsela mafunso awa: Kodi Tony waseŵenzetsa bwanji mafunso mwaluso? Nanga wam’thandiza bwanji mwininyumba kudziŵa bwino moseŵenzetsela mfundo ya pa lemba?

  • Ulendo Wobwelelako: (4 min. olo kucepelapo) Mukayamba makambilano acitsanzo, mwininyumba akambe mawu ofala kwanuko ofuna kukanila ulaliki. Koma mwaluso, loŵelani pa mawu amenewo. (th phunzilo 19)

  • Ulendo Wobwelelako: (5 min. olo kucepelapo) Yambani na makambilano acitsanzo. Gaŵilani bulosha yakuti Uthenga Wabwino na kuyambitsa phunzilo la Baibo pa phunzilo 11. (th phunzilo 9)

UMOYO WATHU WACIKHRISTU

  • Nyimbo 125

  • Zofunikila za Mpingo: (15 min.)

  • Phunzilo la Baibo la Mpingo: (30 min. olo kucepelapo) lfb phunzilo 9, 10

  • Mawu Othela (3 min. olo kucepelapo)

  • Nyimbo 36 na Pemphelo

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani