LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb20 December tsa. 4
  • Phunzilamponi Kanthu pa Malamulo Okhudza Nthenda ya Khate

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Phunzilamponi Kanthu pa Malamulo Okhudza Nthenda ya Khate
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2020
  • Nkhani Zofanana
  • Kodi Mudziŵa?
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yogawila)—2016
  • Mmene Mungasankhile Zosangulutsa Zabwino
    “Khalanibe m’Cikondi ca Mulungu”
  • Mmene Tingasankhile Zosangalatsa
    Mmene Tingakhalilebe mu Cikondi ca Mulungu
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2020
mwb20 December tsa. 4

CUMA COPEZEKA M’MAWU A MULUNGU | LEVITIKO 12-13

Phunzilamponi Kanthu pa Malamulo Okhudza Nthenda ya Khate

13:4, 5, 45, 46, 52, 57

Kodi mfundo zimene panazikidwa malamulo okhudza nthenda ya khate zitiphunzitsa ciani pa nkhani yoteteza umoyo wathu wauzimu?

  • Yehova anaphunzitsa ansembe mmene angaidziŵile mwamsanga nthenda ya khate. Abusa acikhristu masiku ano amacita cangu kuthandiza anthu amene afunika thandizo lauzimu.—Yak. 5:14, 15

  • Aisiraeli anali kuwononga cinthu ciliconse cimene khate lafalikilapo, pofuna kuti lisapitilize kufalikila. Nawonso Akhristu afunika kulolela kuleka kapena kudzimana zinthu zina m’malo molola kuti zinthuzo ziwagwetsele m’chimo. (Mat. 18:8, 9) Zinthu zimenezo zingaphatikizepo zizoloŵezi zoipa, mayanjano, kapena zosangalatsa zoipa

Mayi watsimikiza mtima kuleka umoyo wake wakale. Watembenuka na kulekelatu khalidwe lake lakale la kumwa mwaucidakwa.

Kodi munthu angaonetse bwanji kuti afunitsitsa kulandila thandizo locokela kwa Yehova?

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani