JUNE 24-30
MASALIMO 54-56
Nyimbo 48 na Pemphelo | Mawu Oyamba (Mph. 1)
1. Mulungu Ali Kumbali Yanu
(Mph. 10)
Mofanana na Davide, dalilani Yehova mukacita mantha (Sal. 56:1-4; w06-CN 8/1 22 ¶10-11)
Yehova amayamikila kupilila kwanu ndipo adzakuthandizani (Sal. 56:8; cl-CN 243 ¶9)
Yehova ali kumbali yanu. Iye sadzalola kuti cinthu ciliconse cikuvulazeni kwamuyaya (Sal. 56:9-13; Aroma 8:36-39; w22.06 18 ¶16-17)
2. Kufufuza Cuma Cauzimu
(Mph. 10)
Sal. 55:12, 13—Kodi Yehova anakonzelatu zoti Yudasi akapeleke Yesu? (it-1-E 857-858)
Pa kuŵelenga Baibo kwa mlungu uno, munapeza mfundo zothandiza ziti zimene mungakonde kutigaŵilako?
3. Kuŵelenga Baibo
(Mph. 4) Sal. 55:1-23 (th phunzilo 10)
4. Kuyambitsa Makambilano
(Mph. 3) ULALIKI WAPOYELA. Uzani munthu za pulogilamu yathu yophunzitsa Baibo, ndipo m’patseni kakhadi kopemphela phunzilo la Baibo. (th phunzilo 11)
5. Kubwelelako
(Mph. 4) ULALIKI WAMWAYI. (lmd phunzilo 7 mfundo 4)
6. Nkhani
(Mph. 5) w23.01 29-30 ¶12-14—Mutu: Cikondi Cathu pa Khristu Cimatilimbikitsa Kukhala Olimba Mtima. Onani cithunzi. (th phunzilo 9)
Nyimbo 153
7. Tingakhalebe Okondwela Ngakhale . . . Pa Lupanga
(Mph. 5) Kukambilana.
Tambitsani VIDIYO. Kenako funsani omvela kuti:
Kodi pa zimene zinacitikila m’bale Dugbe mwaphunzilapo ciyani cokuthandizani mukacita mantha?
8. Vidiyo yakuti Zimene Gulu Lakwanitsa Kucita ya June
(Mph. 10) Tambitsani VIDIYO.
9. Phunzilo la Baibo la Mpingo
(Mph. 30) bt mutu 11 ¶11-19