LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb24 May masa. 12-13
  • June 17-23

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • June 17-23
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku Misonkhano—2024
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku Misonkhano—2024
mwb24 May masa. 12-13

JUNE 17-23

MASALIMO 51-53

Nyimbo 89 na Pemphelo | Mawu Oyamba (Mph. 1)

CUMA COPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

1. Zimene Mungacite Kuti Mupewe Macimo Akulu-akulu

(Mph. 10)

Musamadzidalile cifukwa munthu aliyense akhoza kucita zoipa (Sal. 51:5; 2 Akor. 11:3)

Khalani na pulogilamu yabwino yocita zinthu zauzimu nthawi zonse (Sal. 51:6; w19.01 15 ¶4-5)

Pewani maganizo oipa na zilakolako zonyansa (Sal. 51:​10-12; w15 6/15 14 ¶5-6)

Zithunzi: M’bale wacinyamata akutsatila pulogilamu yake yocita zinthu zauzimu. 1. Akuŵelenga Baibo. 2. Akupemphela mocokela pansi pa mtima. 3. Akuyankhapo pa msonkhano. 4. Akutengako mbali mu ulaliki wapoyela.

2. Kufufuza Cuma Cauzimu

(Mph. 10)

  • Sal. 52:​2-4—Kodi mavesiwa akutiuza kuti Doegi anali munthu wotani? (it-1-E 644)

  • Pa kuŵelenga Baibo kwa mlungu uno, munapeza mfundo zothandiza ziti zimene mungakonde kutigaŵilako?

3. Kuŵelenga Baibo

(Mph. 4) Sal. 51:​1-19 (th phunzilo 12)

CITANI KHAMA PA ULALIKI

4. Kuyambitsa Makambilano

(Mph. 2) ULALIKI WAPOYELA. (lmd phunzilo 7 mfundo 3)

5. Kuyambitsa Makambilano

(Mph. 2) KU NYUMBA NA NYUMBA. (lmd phunzilo 4 mfundo 4)

6. Kubwelelako

(Mph. 3) ULALIKI WAMWAYI. Phunzitsani munthuyo dzina la Mulungu. (lmd phunzilo 9 mfundo 5)

7. Kupanga Ophunzila

(Mph. 4) lff phunzilo 14 mfundo 7, komanso mbali yakuti Anthu Ena Amakamba Kuti (lmd phunzilo 11 mfundo 5)

UMOYO WATHU WACIKHRISTU

Nyimbo 115

8. Zimene Mungacite Kuti Mukonze Zolakwa Zanu

(Mph. 15) Kukambilana.

Zithunzi: Zithunzi za m’vidiyo yakuti “Umoyo Wanga Nili Wacinyamata—Kodi Ningakonze Bwanji Zolakwa Zanga?” 1. Thalila. 2. José.

Ngakhale timayesetsa kucita zinthu zoyenela, tonse timalakwitsabe. (1 Yoh. 1:8) Tikalakwa tisalole manyazi kapena mantha oopa cilango kutilepheletsa kupempha Yehova kuti atikhululukile na kutithandiza. (1 Yoh. 1:9) Kupemphela kwa Yehova ndico cinthu coyamba cimene cingatithandize kukonza zolakwa zathu.

Ŵelengani Salimo 51:​1, 2, 17. Kenako funsani omvela kuti:

  • Kodi mawu a Davide amatilimbikitsa bwanji kupemphela kwa Yehova tikacita chimo lalikulu?

Tambitsani VIDIYO YAKUTI Umoyo Wanga Nili Wacinyamata—Kodi Ningakonze Bwanji Zolakwa Zanga? Kenako funsani omvela kuti:

  • Kodi ni zinthu zotani zinapangitsa kuti Thalila na José alakwitse zinthu?

  • Kodi anacita ciyani kuti akonze zolakwa zawo?

  • Kodi kucita zimenezi kunawapindulila bwanji?

9. Phunzilo la Baibo la Mpingo

(Mph. 30) bt mutu 11 ¶5-10, bokosi pa tsa. 89

Mawu Othela (Mph. 3) | Nyimbo 129 na Pemphelo

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani