LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb25 January tsa. 4
  • January 13-19

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • January 13-19
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku Misonkhano—2025
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku Misonkhano—2025
mwb25 January tsa. 4

JANUARY 13-19

MASALIMO 135-137

Nyimbo 2 na Pemphelo | Mawu Oyamba (Mph. 1)

CUMA COPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

Mose watambasula manja ake pogaŵa Nyanja Yofiila. Aisiraeli na gulu la anthu a mitundu yosiyanasiyana akuyang’ana modabwa.

1. “Ambuye Wathu Ndi Wamkulu Kuposa Milungu Ina Yonse”

(Mph. 10)

Yehova waonetsa kuti ali na mphamvu zolamulila cilengedwe conse (Sal. 135:​5, 6; it-2-E 661 ¶4-5)

Iye amateteza anthu ake (Eks. 14:​29-31; Sal. 135:14)

Amatithandiza tikafooka (Sal. 136:23; w21.11 6 ¶16)

2. Kufufuza Cuma Cauzimu

(Mph. 10)

  • Sal. 135:​1, 5​—N’cifukwa ciyani mawu akuti “Ya” amaseŵenzetsedwa kaŵili-kaŵili m’Baibo? (it-1-E 1248)

  • Pa kuŵelenga Baibo kwa mlungu uno, munapeza mfundo zothandiza ziti zimene mungakonde kutifotokozelako?

3. Kuŵelenga Baibo

(Mph. 4) Sal. 135:​1-21 (th phunzilo 11)

CITANI KHAMA PA ULALIKI

4. Kuyambitsa Makambilano

(Mph. 3) ULALIKI WAMWAYI. Patsanani mafoni namba na munthu amene waonetsa cidwi. (lmd phunzilo 2 mfundo 4)

5. Kubwelelako

(Mph. 4) KU NYUMBA NA NYUMBA. Muitanileni ku misonkhano. (lmd phunzilo 9 mfundo 4)

6. Kufotokoza Zimene Mumakhulupilila

(Mph. 5) Citsanzo. ijwfq nkhani 7​—Mutu: Kodi Mboni za Yehova ni Akhristu? (th phunzilo 12)

UMOYO WATHU WACIKHRISTU

Nyimbo 10

7. Zofunikila za Mpingo

(Mph. 15)

8. Phunzilo la Baibo la Mpingo

(Mph. 30) bt mutu 21 ¶1-7, bokosi pa tsa. 166

Mawu Othela (Mph. 3) | Nyimbo 90 na Pemphelo

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani