LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb25 March tsa. 10
  • April 7-13

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • April 7-13
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku Misonkhano—2025
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku Misonkhano—2025
mwb25 March tsa. 10

APRIL 7-13

MIYAMBO 8

Nyimbo 89 ndi Pemphelo | Mawu Oyamba (Mph. 1)

CUMA COPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

Yesu akuphunzitsa anthu panja.

1. Mvelani Yesu Amene Amachedwa Nzelu

(Mph. 10)

Yesu, amene amachedwa nzelu m’buku la Miyambo, ndiye anali “woyamba kulengedwa ndi Yehova” (Miy. 8:​1, 4, 22; cf-CN 131 ¶7)

Nzelu za Yesu komanso cikondi cake pa Atate wake zinakula panthawi yonse imene anakhala ndi Yehova polenga zinthu (Miy. 8:​30, 31; cf-CN 131-132 ¶8-9)

Timapindula ndi nzelu za Yesu tikamamumvela (Miy. 8:​32, 35; w09-CN 4/15 31 ¶14)

2. Kufufuza Cuma Cauzimu

(Mph. 10)

  • Miy. 8:​1-3​—Kodi nzelu imangokhalila “kufuula mokweza” m’lingalilo lotani? (g-CN 5/14 16)

  • Pa kuwelenga Baibulo kwa mlungu uno, munapeza mfundo zothandiza ziti zimene mungakonde kutifotokozelako?

3. Kuwelenga Baibulo

(Mph. 4) Miy. 8:​22-36 (th phunzilo 10)

CITANI KHAMA PA ULALIKI

4. Kubwelelako

(Mph. 4) ULALIKI WAMWAYI. Yankhani mafunso okhudza zimene zidzacitika pa Cikumbutso omwe munthu amene akufuna kukapezekapo angakhale nawo. (lmd phunzilo 9 mfundo 3)

5. Kuyambitsa Makambilano

(Mph. 3) ULALIKI WAMWAYI. Cikumbutso cisanayambe landilani munthu amene wabwela cifukwa anapeza kapepala kaciitano pakhomo pake. Pulogilamu ikatha yankhani mafunso amene angakhale nawo. (lmd phunzilo 3 mfundo 5)

6. Kufotokoza Zimene Mumakhulupilila

(Mph. 5) Nkhani. ijwbq nkhani 160​—Mutu: N’cifukwa Ciyani Baibulo Limati Yesu Ndi Mwana wa Mulungu? (th phunzilo 1)

UMOYO WATHU WACIKHRISTU

Nyimbo 105

7. Zofunikila za Mpingo

(Mph. 15)

8. Phunzilo la Baibulo la Mpingo

(Mph. 30) bt mutu 25 ¶1-4, bokosi pa tsa. 199

Mawu Othela (Mph. 3) | Nyimbo 7 ndi Pemphelo

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani