LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb25 July masa. 2-3
  • July 7-13

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • July 7-13
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku Misonkhano—2025
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku Misonkhano—2025
mwb25 July masa. 2-3

JULY 7-13

MIYAMBO 21

Nyimbo 98 ndi Pemphelo | Mawu Oyamba (Mph. 1)

CUMA COPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

1. Malangizo Anzelu Othandiza Kuti Ukwati Ukhale Wacimwemwe

(Mph. 10)

Musafulumile kukwatilana ndi munthu musanamudziwe bwino (Miy. 21:5; w03-CN 10/15 4 ¶5)

Muzikhala odzicepetsa pakabuka mikangano (Miy. 21:​2, 4; g-CN 7/08 7 ¶2)

Muzicitilana zinthu moleza mtima komanso mokoma mtima (Miy. 21:19; w06-CN 9/15 28 ¶13)

Mwamuna akumvetsela moleza mtima pamene mkazi wake akumufotokozela maganizo ake.

2. Kufufuza Cuma Cauzimu

(Mph. 10)

  • Miy. 21:31​—Kodi vesili litithandiza bwanji kumvetsa ulosi wa pa Chivumbulutso 6:2? (w05-CN 1/15 17 ¶9)

  • Pa kuwelenga Baibo kwa mlungu uno, munapeza mfundo zothandiza ziti zimene mungakonde kutifotokozelako?

3. Kuwelenga Baibo

(Mph. 4) Miy. 21:1-18 (th phunzilo 5)

CITANI KHAMA PA ULALIKI

4. Kuyambitsa Makambilano

(Mph. 3) KUNYUMBA NDI NYUMBA. (lmd phunzilo 3 mfundo 3)

5. Kubwelelako

(Mph. 4) ULALIKI WAMWAYI. (lmd phunzilo 7 mfundo 3)

6. Kufotokoza Zimene Mumakhulupilila

(Mph. 5) Citsanzo. ijwfq nkhani 54​—Mutu: Kodi a Mboni za Yehova Amaiona Bwanji Nkhani Yothetsa Ukwati? (lmd phunzilo 4 mfundo 3)

UMOYO WATHU WACIKHRISTU

Nyimbo 132

7. Muzilemekeza Mnzanu wa mu Ukwati

(Mph. 15) Kukambilana.

Cithunzi ca mu vidiyo yakuti “Kuti Banja Likhale Lacimwemwe: Onetsani Ulemu.” Mlongo wabweletsela mwamuna wake kapu ya zakumwa pamene akuwelenga pa mpando.

Pa tsiku la ukwati, munalumbila pamaso pa Yehova kuti mudzamukonda mnzanu wa mu ukwati ndi kumulemekeza. Conco mmene mumacitila zinthu ndi mwamuna wanu kapena mkazi wanu zimakhudza ubale wanu ndi Yehova.​—Miy. 20:25; 1 Pet. 3:7.

Tambitsani VIDIYO yakuti Kuti Banja Likhale Lacimwemwe: Onetsani Ulemu. Kenako funsani omvela kuti:

  • N’cifukwa ciyani kulemekeza mnzanu wa mu ukwati n’kofunika?

  • Kodi mungafunike kupanga masinthidwe otani kuti muzilemekezana kwambili?

  • Kodi ndi mfundo za m’Baibo ziti zimene zingakuthandizeni?

  • Kodi mungaonetse ulemu kwa mnzanu wa mu ukwati m’njila ziti?

  • Kodi muyenela kumaganizila zinthu ziti zimene mnzanu wa mu ukwati amacita, ndipo n’cifukwa ciyani?

8. Phunzilo la Baibo la Mpingo

(Mph. 30) bt mutu 28 ¶16-22

Mawu Othela (Mph. 3) | Nyimbo 72 ndi Pemphelo

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani