LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb25 September tsa. 16
  • October 27–November 2

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • October 27–November 2
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku Misonkhano—2025
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku Misonkhano—2025
mwb25 September tsa. 16

OCTOBER 27–NOVEMBER 2

MLALIKI 11-12

Nyimbo 155 ndi Pemphelo | Mawu Oyamba (Mph. 1)

CUMA COPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

1. Mmene Mungakhalile Athanzi Komanso Acimwemwe

(Mph. 10)

Ngati n’zotheka, muzipeza nthawi yoothela dzuwa komanso kamphepo kayaziyazi (Mlal. 11:​7, 8; g-CN 3/15 13 ¶6-7)

Muzisamalila thanzi lanu (Mlal. 11:10; w23.02 21 ¶6-7)

Koposa zonse, muzilambila Yehova ndi mtima wonse (Mlal. 12:13; w24.09 2 ¶2-3)

Mwamuna ndi mkazi wake omwe ndi okalamba, mosangalala akugwilila nchito limodzi m’dimba.

2. Kufufuza Cuma Cauzimu

(Mph. 10)

  • Mlal. 12:​9, 10​—Kodi lembali litiphunzitsa ciyani za anthu amene Mulungu anagwilitsa nchito kulemba Baibo? (it-E “Kuuzilidwa” ¶10)

  • Pa kuwelenga Baibo kwa mlungu uno, munapeza mfundo zothandiza ziti zimene mungakonde kutifotokozelako?

3. Kuwelenga Baibo

(Mph. 4) Mlal. 12:​1-14 (th phunzilo 12)

CITANI KHAMA PA ULALIKI

4. Kubwelelako

(Mph. 3) KUNYUMBA NDI NYUMBA. (lmd phunzilo 8 mfundo 3)

5. Kubwelelako

(Mph. 4) ULALIKI WAMWAYI. Pa makambilano apita, munthuyo anakuuzani kuti posacedwa anatayikilidwa wokondedwa wake mu imfa. (lmd phunzilo 9 mfundo 3)

6. Nkhani

(Mph. 5) lmd zakumapeto A mfundo 13​—Mutu: Mulungu Amafuna Kutithandiza. (th phunzilo 20)

UMOYO WATHU WACIKHRISTU

Nyimbo 111

7. Zofunikila za Mpingo

(Mph. 15)

8. Phunzilo la Baibo la Mpingo

(Mph. 30) rr mutu 5 ¶17-22 ndi bokosi 5A

Mawu Othela (Mph. 3) | Nyimbo 127 ndi Pemphelo

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani