LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb25 November tsa. 16
  • December 29, 2025–January 4, 2026

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • December 29, 2025–January 4, 2026
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku Misonkhano—2025
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku Misonkhano—2025
mwb25 November tsa. 16

DECEMBER 29, 2025–JANUARY 4, 2026

YESAYA 14-16

Nyimbo 63 ndi Pemphelo | Mawu Oyamba (Mph. 1)

CUMA COPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

1. Adani a Anthu a Mulungu Adzalangidwa

(Mph. 10)

Babulo amene anali wodzikuza anali kudzawonongedwa kothelatu (Yes. 14:​13-15, 22, 23; ip-1-CN 180 ¶16; 184 ¶24)

Yehova ananenelatu kuti adzaphwanya Msuri m’dziko lake (Yes. 14:​24, 25; ip-1-CN 189 ¶1)

Yehova anatinso adzacititsa manyazi ulemelelo wa Mowabu (Yes. 16:​13, 14; ip-1-CN 194 ¶12)

Zithunzi: 1. Zipupa komanso geti lolowela za mzinda wakale wa Babulo. 2. Matongwe za Mzinda wa Babulo masiku ano.

Left: C. Sappa/DeAgostini via Getty Images; right: Image © Homo Cosmicos/Shutterstock

2. Kufufuza Cuma Cauzimu

(Mph. 10)

  • Yes. 14:​1, 2​—Lembali lati anthu a Yehova “adzagwila anthu amene anawagwila n’kupita nawo kudziko lina.” Kodi zimenezi zinacitika bwanji? (w06-CN 12/1 10 ¶11)

  • Pa kuwelenga Baibo kwa mlungu uno, munapeza mfundo zothandiza ziti zimene mungakonde kutifotokozelako?

3. Kuwelenga Baibo

(Mph. 4) Yes. 16:​1-14 (th phunzilo 10)

CITANI KHAMA PA ULALIKI

4. Kuyambitsa Makambilano

(Mph. 3) KUNYUMBA NDI NYUMBA. (lmd phunzilo 2 mfundo 5)

5. Kubwelelako

(Mph. 4) ULALIKI WAPOYELA. (lmd phunzilo 9 mfundo 4)

6. Nkhani

(Mph. 5) ijwbq nkhani 108—Mutu: Kodi Ulosi N’ciyani? (th phunzilo 14)

UMOYO WATHU WACIKHRISTU

Nyimbo 2

7. Zofunikila za Mpingo

(Mph. 15)

8. Phunzilo la Baibo la Mpingo

(Mph. 30) rr mutu 8 ¶8-15 ndi bokosi 8A

Mawu Othela (Mph. 3) | Nyimbo 16 ndi Pemphelo

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani