LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • w15 12/15 masa. 1-2
  • Zamkati

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Zamkati
  • Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova—2015
  • Tumitu
  • NKHANI ZOPHUNZILA
  • NKHANI ZOPHUNZILA
  • NKHANI ZINA M’MAGAZINI INO
Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova—2015
w15 12/15 masa. 1-2

Zamkati

December 15, 2015

© 2015 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania

NKHANI ZOPHUNZILA

FEBRUARY 1-7, 2016

Yehova Mulungu Amakonda Kukamba ndi Anthu

TSAMBA 3

FEBRUARY 8-14, 2016

Baibulo Lomasulidwa Bwino Kwambili

TSAMBA 9

FEBRUARY 15-21, 2016

Gwilitsilani Nchito Bwino Lilime Lanu

TSAMBA 17

FEBRUARY 22-28, 2016

Yehova Adzakucilikizani

TSAMBA 23

NKHANI ZOPHUNZILA

▪ Yehova Mulungu Amakonda Kukamba ndi Anthu

▪ Baibulo Lomasulidwa Bwino Kwambili

Kwa zaka zambili, Yehova wakhala akukamba momasuka ndi atumiki ake m’zinenelo zosiyanasiyana. Tikambilana zimenezi m’nkhani ziŵilizi, ndipo tiphunzilanso mmene Baibulo la Dziko Latsopano lathandizila anthu kulemekeza dzina la Mulungu ndi kudziŵa cifunilo cake.

▪ Gwilitsilani Nchito Bwino Lilime Lanu

Kulankhula ndi mphatso yocokela kwa Mulungu. Nkhaniyi ifotokoza cifukwa cake tiyenela kudziŵa nthawi yabwino yokamba zinthu, zimene tiyenela kukamba, ndi mmene tiyenela kuzikambila. Itilimbikitsanso kutengela Yesu mwa kugwilitsila nchito mphatsoyi polemekeza Mulungu ndi kulimbikitsa ena.

▪ Yehova Adzakucilikizani

Tonse timadwala. Koma kodi tiyenela kuyembekezela kuti Yehova adzaticilitsa mozizwitsa monga mmene anacilitsila anthu akale? N’ciani cimene tiyenela kukumbukila munthu wina akatipatsa malangizo okhudza thanzi? Nkhaniyi iyankha mafunso amenewa ndi kutithandiza kupanga zosankha zabwino.

NKHANI ZINA M’MAGAZINI INO

15 Muziyamikila Kuolowa Manja kwa Yehova

29 Ndili pa Mtendele ndi Mulungu Komanso ndi Amai

PACIKUTO: Mpainiya wapadela akulalikila uthenga wabwino mosangalala kwa mai ndi ana ake. Mboni za Yehova zimalalikila coonadi m’Cisipanishi ndi m’Ciguarani. Izi ndi zinenelo zimene zimakambidwa ndi anthu ambili m’dzikoli

PARAGUAY

KULI ANTHU

6,800,236

OFALITSA

9,760

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani