LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • w16 March tsa. 2
  • Zamkati

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Zamkati
  • Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2016
Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2016
w16 March tsa. 2

Zamkati

3 Kodi Mungathandize Ena Mumpingo Wanu?

MLUNGU WA MAY 2-8, 2016

6 Acinyamata​—Kodi Ndinu Okonzeka Kubatizidwa?

MLUNGU WA MAY 9-15, 2016

12 Acinyamata​—Kodi Mungakonzekele Bwanji Ubatizo?

Atumiki a Yehova ndife osangalala kwambili cifukwa caka ciliconse anthu oposa 250,000 amabatizidwa. Ambili amene amapanga cosankha cimeneci ndi acinyamata, ndipo ena amakhala kuti sanakwanitse zaka 13. N’ciani cinawathandiza kudziŵa kuti tsopano ndi okonzeka kubatizidwa? Kodi anakonzekela bwanji ubatizo? Nkhani ziŵilizi zidzayankha mafunso amenewa.

MLUNGU WA MAY 16-22, 2016

18 Kodi Tingalimbitse Bwanji Mgwilizano Pakati Pathu?

Yehova amatidalitsa ngati tigwilizana pocita cifunilo cake. Nkhaniyi ili ndi mfundo zimene zingatithandize kuti tizigwilizana m’banja, mumpingo, ndiponso polalikila

MLUNGU WA MAY 23-29, 2016

24 Yehova Amatsogolela Anthu Ake m’Njila ya ku Moyo

Nthawi zonse, Yehova amatsogolela anthu ake. Nkhaniyi, ifotokoza mmene Mulungu anali kupatsila anthu ake malangizo ndi malamulo atsopano nthawi zonse zinthu zikasintha. Tidzaphunzilanso zimene zingatithandize kuti tizidalila citsogozo ca Yehova.

29 Mafunso Ocokela kwa Aŵelengi

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani