LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • w16 April tsa. 2
  • Zamkati

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Zamkati
  • Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2016
Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2016
w16 April tsa. 2

Zamkati

MLUNGU WA MAY 30, 2016–JUNE 5, 2016

3 Mulungu Amakonda Anthu Okhulupilika

Nkhaniyi ifotokoza cimene cinathandiza Yefita ndi mwana wake wamkazi kukhalabe okhulupilika ngakhale panthawi yovuta. Tidzaphunzila cifukwa cake tifunika kudzipeleka kwa Mulungu kuti apitilize kutikonda.

MLUNGU WA JUNE 6-12, 2016

9 “Mulole Kuti Kupilila Kumalize Kugwila Nchito Yake”

Kuti tidzalandile mphatso ya moyo wosatha, tiyenela kupilila mpaka mapeto. Nkhaniyi ifotokoza zinthu zinai zimene zingatithandize kupilila, ndiponso zitsanzo zitatu za anthu okhulupilika amene anapilila. Ifotokozanso nchito imene khalidwe la kupilila liyenela kumaliza mwa aliyense wa ife.

MLUNGU WA JUNE 13-19, 2016

15 N’cifukwa Ciani Tiyenela Kusonkhana?

Pali zinthu zambili zimene zingatilepheletse kusonkhana nthawi zonse. Nkhaniyi itilimbikitsa kuti tipitilize kupezeka pamisonkhano. Ifotokoza cifukwa cake kupezeka pamisonkhano kumatipindulitsa, kumathandiza ena, ndi kukondweletsa Yehova.

MLUNGU WA JUNE 20-26, 2016

21 Pewani Kutenga Mbali m’Ndale za Dziko Loipali

Ngakhale kuti maboma ambili masiku ano amatilola kusatenga mbali m’ndale, tiyenela kuyembekezela kuti adzatikakamiza kutengamo mbali pamene tiyandikila mapeto. M’nkhani ino, tikambilana zinthu zinai zimene zidzatithandiza kukhalabe okhulupilika kwa Yehova.

27 Mbili Yanga​—Masisitele Anakhala Paubale Weniweni Wakuuzimu

31 Kodi Utumiki Wanu Uli Ngati Mame?

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani