LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • w16 April tsa. 1
  • Yophunzila

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Yophunzila
  • Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2016
Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2016
w16 April tsa. 1
Nsanja ya Mlonda Yophunzila ya April 2016

Yophunzila

APRIL 2016

NKHANI ZOPHUNZILA MLUNGU WA: MAY 30–JUNE 26, 2016

© 2016 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania

CITHUNZI CA PACIKUTO:

COLOMBIA

Mboni zimacita zimene zingathe kuti zilalikile uthenga wabwino kwa anthu amene amakamba Ciwayu. Anthu amenewa amakonda kukamba za Mulungu. Nthawi zambili amapita kumzinda kukagulitsa zinthu zokongola zimene amapanga. Kumeneko amamva uthenga wabwino kwa Mboni zimene zimacita ulaliki wa poyela

OFALITSA

166,049

MAPHUNZILO A BAIBULO

229,723

OPEZEKA PA CIKUMBUTSO (2015)

510,217

Magazini iyi si yogulitsa. Colinga cake ndi kuthandiza pa nchito yophunzitsa Baibulo imene imacitika padziko lonse lapansi. Ndalama zoyendetsela nchitoyi ndi zimene anthu amapeleka mwa kufuna kwao.

Ngati mufuna kupeleka ndalama zocilikizila nchitoyi, pitani pa www.pr2711.com.

Baibulo limene taseŵenzetsa ndi Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika, kusiyapo ngati taonetsa lina. Komabe, masipeling’i a Cinyanja m’buku lino tatsatila malamulo a m’buku lochedwa A Unified Standard Orthography for South-Central African Languages.

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani