LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • g18 na. 3 tsa. 16
  • M’magazini Ino Thandizo Kwa Ofedwa

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • M’magazini Ino Thandizo Kwa Ofedwa
  • Galamuka!—2018
  • Nkhani Zofanana
  • Zamkati
    Galamuka!—2018
  • Mawu oyamba
    Galamuka!—2018
  • Zimene Mungayembekezele
    Galamuka!—2018
  • Kuŵaŵa Kwa Imfa
    Galamuka!—2018
Onaninso Zina
Galamuka!—2018
g18 na. 3 tsa. 16
Mwamuna wofedwa apeza citonthozo mwa kuŵelenga magazini ino ya Galamuka!

THANDIZO KWA OFEDWA

M’magazini Ino Thandizo Kwa Ofedwa

  • KUŴAŴA KWA IMFA

    Kodi umoyo umakhala bwanji munthu akafedwa? N’cifukwa ciani anthu ofedwa afunika citonthozo?

  • ZIMENE MUNGAYEMBEKEZELE

    Nkhani iyi, ifotokoza maganizo amene anthu amakhala nawo ponena za cisoni, komanso zimene ambili amacita akafedwa. Ngati munafedwa, dziŵani kuti anthu amalila malilo mosiyana-siyana, ndipo zonsezo n’cibadwa.

  • ZIMENE MUNGACITE PALIPANO MUKAFEDWA

    Kodi mungatsatile njila ziti zimene zingakuthandizeni kupilila cisoni? Nkhani iyi, ipeleka malingalilo acindunji amene athandiza ena, ndipo ni ozikidwa pa nzelu zimene n’zothandiza nthawi zonse.

  • THANDIZO LODALILIKA KWAMBILI KWA OFEDWA

    Onani gwelo la citonthozo limene ambili apeza panthawi yovuta kwambili, komanso onani mmene ingakuthandizileni.

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani