LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • sn nyimbo 77
  • Muzikhululuka

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Muzikhululuka
  • Imbirani Yehova
  • Nkhani Zofanana
  • Khalani Wokhululuka
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • “Yehova Anakukhululukilani ndi Mtima Wonse”
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova—2013
  • Yehova Amadalitsa Amene Amakhululukila Anzawo
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2022
  • Tingatengele Bwanji Kukhululuka kwa Yehova?
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2025
Onaninso Zina
Imbirani Yehova
sn nyimbo 77

Nyimbo 77

Muzikhululuka

(Salimo 86:5)

1. Mwachikondi M’lungu

Mwa Yesu anakonza

Kuti tikhululukidwe

Ndi kuthetsadi imfa.

Ngati tilidi olapa,

Ndipo titamupempha,

Pogwiritsa ntchito

Dipo Atikhululukira.

2. Ngati titsanzira

Mulungu wakumwamba

Kukhululukira ena

Tidzakhululukidwa.

Tikhale ololerana,

Tisakhale odana

Koma olemekezana

Komanso okondana.

3. Tikhale n’chifundo,

Chidzatithandizadi

Kusasunga chakukhosi

Kapenanso chidani.

Tikatsanzira Yehova

Maka chikondi chake

Tidzakhululukirana

Tidzafanana naye.

(Onaninso Mat. 6:12; Aef. 4:32; Akol. 3:13.)

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani