LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • sn nyimbo 83
  • Tifunika Kukhala Odziletsa

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Tifunika Kukhala Odziletsa
  • Imbirani Yehova
  • Nkhani Zofanana
  • Kudziletsa N’kofunika
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Kudziletsa—N’kofunika Kuti Tikondweletse Yehova
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2020
  • Phunzilani Kukhala Wodziletsa
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2017
Imbirani Yehova
sn nyimbo 83

Nyimbo 83

Tifunika Kukhala Odziletsa

(Aroma 7:14-25)

1. Timakonda Yehova kwambiri

Koma ndife anthu ochimwa zedi

Choterotu ndi kofunika

Kuti tikhale odziletsa.

2. Satana ndi matupi ochimwa

Tsiku lililonse amatiyesa.

Koma tikadalira M’lungu

Adzateteza mtima wathu.

3. Tanyamula dzina la Yehova

Choncho tisapezeredwe chifukwa.

Pa chilichonse timachita

Tikhale anthu odziletsa.

(Onaninso 1 Akor. 9:25; Agal. 5:23; 2 Pet. 1:6.)

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani