LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 121
  • Kudziletsa N’kofunika

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Kudziletsa N’kofunika
  • ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Nkhani Zofanana
  • Tifunika Kukhala Odziletsa
    Imbirani Yehova
  • Kudziletsa—N’kofunika Kuti Tikondweletse Yehova
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2020
  • Phunzilani Kukhala Wodziletsa
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2017
‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
sjj nyimbo 121

NYIMBO 121

Kudziletsa N’kofunika

Yopulinta

(Aroma 7:14-25)

  1. 1. Ise tikonda Yehova M’lungu.

    Komabe tidziŵa ndise ocimwa.

    Mtima ungatisoceletse.

    Tifunikila kudziletsa.

  2. 2. Tsiku na tsiku timayesedwa

    Kuti’se ticite zinthu zoipa.

    Koma mwa Mau ake M’lungu

    Atithandiza kupambana.

  3. 3. Timaimila dzina la M’lungu,

    Conco, tizipewa kulitonzetsa.

    Mu zocita na m’mau athu,

    Tikhale anthu odziletsa.

(Onaninso 1 Akor. 9:25; Agal. 5:23; 2 Pet. 1:6.)

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani