LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • sn nyimbo 78
  • Kuleza Mtima

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Kuleza Mtima
  • Imbirani Yehova
  • Nkhani Zofanana
  • “Khalani Oleza Mtima”
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Mphatso Yochokera kwa Mulungu ya Mzimu Woyera
    Imbirani Yehova
Imbirani Yehova
sn nyimbo 78

Nyimbo 78

Kuleza Mtima

(Agalatiya 5:22)

1. Yehova Mbuye wathu

Amakonda dzina lake.

Amafunitsitsadi

Kuti lisamanyozedwe.

Kwanthawi yaitali

Wakhala ’kupirira.

Iyetu sanatope

Amaleza mtima.

Anthu m’mitundu yonse

Amafuna ’pulumuke.

Kuleza kwake mtima

Sikudzapita pachabe.

2. Kuti tisapatuke

Tikhale oleza mtima.

Tidzapeza mtendere

N’kupewa kumangokwiya.

Pochita ndi anzathu

Tidzaona zabwino,

N’kukhala odziletsa

Ngakhale m’mavuto.

Kuleza mtima kwathu

Ndiko kudzatithandiza

Kutsanzira Mulungu

Amene tikumudziwa.

(Onaninso Eks. 34:14; Yes. 40:28; 1 Akor. 13:4, 7; 1 Tim. 2:4.)

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani