LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 114
  • “Khalani Oleza Mtima”

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • “Khalani Oleza Mtima”
  • ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Nkhani Zofanana
  • Kuleza Mtima
    Imbirani Yehova
  • Kuleza Mtima Kumatanthauza Kupilila Tili na Colinga
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2018
  • Khalanibe Oleza Mtima
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2023
‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
sjj nyimbo 114

NYIMBO 114

“Khalani Oleza Mtima”

Yopulinta

(Yakobo 5:8)

  1. 1. Yehova Mbuye wathu

    Amakonda dzina lake.

    Iye afunitsitsa

    Kuti lisamanyozedwe.

    Kucokela kalelo

    Iye apililabe.

    Yehova sanatope,

    Amaleza mtima.

    Afuna kuti anthu

    Onse akapulumuke.

    Kuleza mtima kwake

    Sikudzapita pacabe.

  2. 2. Tifunika kukhala

    Oleza mtima kwa onse.

    Tidzapeza mtendele

    Ndipo tidzapewa mkwiyo.

    Tidzapewa kuona

    Zoipa mwa anzathu.

    Tikhale odziletsa

    Olo pa mavuto.

    Titengele Yehova

    Tikhale oleza mtima.

    Ise tikayesetsa

    Tidzapeza madalitso.

(Onaninso Eks. 34:14; Yes. 40:28; 1 Akor. 13:4, 7; 1 Tim. 2:4.)

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani