LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 56
  • Khulupilila Coonadi Iwe Mwini

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Khulupilila Coonadi Iwe Mwini
  • ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Nkhani Zofanana
  • Inuyo Panokha Muzikonda Kwambiri Choonadi
    Imbirani Yehova
  • Khalani ndi Moyo Wopambana
    Imbirani Yehova
  • Umoyo wa Mpainiya
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Aphunzitseni Kucilimika
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
Onaninso Zina
‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
sjj nyimbo 56

NYIMBO 56

Khulupilila Coonadi Iwe Mwini

Yopulinta

(Miyambo 3:1, 2)

  1. 1. Njila yabwino ni njila ya co’nadi,

    Palibe angakusankhile.

    Mvela uphungu wocokela kwa M’lungu,

    Ndipo um’khulupilile.

    (KOLASI)

    Panga co’nadi

    Cikhale cako-cako.

    Ndipo Yehova

    ‘dzakudalitsa,

    Udzapeza cimwemwe.

  2. 2. Zonse zabwino zimene umacita

    Potumikila M’lungu wathu,

    Udzapezadi madalitso ambili,

    Inde, moyo wamuyaya.

    (KOLASI)

    Panga co’nadi

    Cikhale cakocako.

    Ndipo Yehova

    ‘dzakudalitsa,

    Udzapeza cimwemwe.

  3. 3. Kuli Yehova ndise ana ang’ono

    Ofunika kulangizidwa.

    Ukayenda na Atate wakumwamba

    Udzapeza madalitso.

    (KOLASI)

    Panga co’nadi

    Cikhale cakocako.

    Ndipo Yehova

    ‘dzakudalitsa,

    Udzapeza cimwemwe.

(Onaninso Sal. 26:3; Miy. 8:35; 15:31; Yoh. 8:31, 32)

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani