LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • CO-pgm21 masa. 4-5
  • Tsiku Laciŵili

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Tsiku Laciŵili
  • Pulogilamu ya Msonkhano Wacigawo wa mu 2021
  • Nkhani Zofanana
  • Tsiku Laciŵili
    Pulogilamu ya Msonkhano Wacigawo wa mu 2020
  • Tsiku Loyamba
    Pulogilamu ya Msonkhano Wacigawo wa mu 2024
  • Tsiku Lacitatu
    Pulogilamu ya Msonkhano Wacigawo wa mu 2021
  • Tsiku Laciŵili
    Pulogilamu ya Msonkhano Wacigawo wa mu 2019
Onaninso Zina
Pulogilamu ya Msonkhano Wacigawo wa mu 2021
CO-pgm21 masa. 4-5
Zithunzi: 1. Mlongo akukambilana na mwana wake wamwamuna na wamkazi. 2. Alongo aŵili akulalikila m’dela la kumudzi ku Asia. 3. Danieli na anzake atatu aciheberi aimilila pamaso pa mfumu ya Babulo.

Tsiku Laciŵili

‘Menyani mwamphamvu nkhondo ya cikhulupililo’​—Yuda 3

M’MAŴA

  • 9:20 Vidiyo ya Nyimbo

  • 9:30 Nyimbo Na. 57 na Pemphelo

  • 9:40 YOSIYILANA: Kumbukilani​—Anthu Opanda Cikhulupililo Angapeze Cikhulupililo!

    • • Anineve (Yona 3:5)

    • • Abale a Yesu Akuthupi (1 Akorinto 15:7)

    • • Anthu Ochuka (Afilipi 3:7, 8)

    • • Anthu Osapembedza (Aroma 10:13-15; 1 Akorinto 9:22)

  • 10:30 Mangani Cikhulupililo mwa Kuseŵenzetsa Buku Lakuti, Kondwelani na Moyo Kwamuyaya! (Yohane 17:3)

  • 10:50 Nyimbo Na. 67 na Zilengezo

  • 11:00 YOSIYILANA: Omenya Nkhondo ya Cikhulupililo Mwacipambano

    • • Aja Amene Mnzawo wa m’Cikwati si Mboni (Afilipi 3:17)

    • • Amene Akuleledwa na Kholo Limodzi (2 Timoteyo 1:5)

    • • Akhristu Amene Sali Pabanja (1 Akorinto 12:25)

  • 11:45 UBATIZO: Pokhala na Cikhulupililo, Tidzapeza Moyo Wosatha! (Mateyu 17:20; Yohane 3:16; Aheberi 11:6)

  • 12:15 Nyimbo Na. 79 na Kupumula

MASANA

  • 13:35 Vidiyo ya Nyimbo

  • 13:45 Nyimbo Na. 24

  • 13:50 YOSIYILANA: Mmene Abale Athu Akuonetsela Cikhulupililo . . .

    • • mu Africa

    • • ku Asia

    • • ku Europe

    • • ku North America

    • • ku Oceania

    • • ku South America

  • 14:15 YOSIYILANA: Loŵani Pakhomo la Zocita Zambili m’Cikhulupililo

    • • Phunzilani Cinenelo Catsopano (1 Akorinto 16:9)

    • • Katumikilenkoni Kumalo Osoŵa (Aheberi 11:8-10)

    • • Funsilani Kuloŵa Sukulu ya Alengezi a Ufumu (1 Akorinto 4:17)

    • • Dzipelekeni Kukathandiza pa Nchito Zomanga za Gulu (Nehemiya 1:2, 3; 2:5)

    • • ‘Ikani Kenakake Pambali’ Kothandizila pa Nchito ya Yehova (1 Akorinto 16:2)

  • 15:15 Nyimbo Na. 84 na Zilengezo

  • 15:20 SEŴELO LA M’BAIBO: Danieli: Citsanzo Cokhala Wokhulupilika kwa Moyo Wonse— Gawo 1 (Danieli 1:1–2:49; 4:1-33)

  • 16:20 ‘Menyani Mwamphamvu Nkhondo ya Cikhulupililo’! (Yuda 3; Miyambo 14:15; Aroma 16:17)

  • 16:55 Nyimbo Na. 38 na Pemphelo Lothela

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani