LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • km 4/15 tsa. 4
  • Maulaliki Acitsanzo

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Maulaliki Acitsanzo
  • Utimiki Wathu wa Ufumu—2015
  • Nkhani Zofanana
  • Maulaliki Acitsanzo
    Utimiki Wathu wa Ufumu—2015
  • Maulaliki Acitsanzo
    Utimiki Wathu wa Ufumu—2013
Utimiki Wathu wa Ufumu—2015
km 4/15 tsa. 4

Maulaliki Acitsanzo

NSANJA YA MLONDA March-April

“Anthu ena sadziŵa kuti m’Baibulo muli malangizo amene angawathandize pa nchito imene amagwila. Onani zimene vesi ili limanena. [Ŵelengani Mlaliki 3:12] Magazini iyi ikufotokoza mfundo za m’Baibulo zimene zingakuthandizeni kupeza cimwemwe pa nchito yanu. Kodi mungakonde kuliŵelenga?”

Galamukani! May

“Kodi muganiza kuti n’zotheka kukhala m’dziko lopanda umphawi komanso mmene anthu adzakhala ndi nyumba zabwino? [Yembekezani yankho.] Onani zimene Mulungu watilonjeza pa nkhani imeneyi. [Ŵelengani Yesaya 65:21-22.] Galamukani! iyi ifotokoza mmene Mulungu adzakwanilitsila cifunilo cake kwa anthu pa dziko ndi zimene ife tingacite kuti tidzakhalemo.”

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani