LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb16 June tsa. 7
  • “Umutulile Yehova Nkhawa Zako”

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • “Umutulile Yehova Nkhawa Zako”
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Msonkhano (2016)
  • Nkhani Zofanana
  • Mmene Tingathanilane Nazo Nkhawa
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2022
  • “Mulungu Ndiye Mthandizi Wanga”
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Msonkhano (2016)
  • Tulila Yehova Nkhawa Zako
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Tulilani Yehova Nkhawa Zanu Zonse
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2016
Onaninso Zina
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Msonkhano (2016)
mwb16 June tsa. 7

CUMA COPEZEKA M’MAU A MULUNGU | MASALIMO 52-59

“Umutulile Yehova Nkhawa Zako”

Davide anakumana ndi mavuto ambili. Pamene Salimo 55 inali kulembedwa, iye anali atakumanapo kale ndi mavuto monga . . .

  • Goliyati ndi wanchito wake

    Kunyozedwa

  • Davide alewa mkondo

    Kuzunzidwa

  • Davide avutika kwambili cifukwa codziimba mlandu

    Kudziimba mlandu

  • Batiseba alila

    Mavuto a m’banja

  • Davide ni wodwala pabedi yake

    Kudwala

  • Davide acitilidwa zinthu mopanda cilungamo

    Kucitilidwa zinthu mopanda cilungamo

Ngakhale kuti mavuto a Davide anaoneka ngati ndi osapililika, iye anawapililabe. Anthu amene aona kuti sangapilile mavuto, angatsatile malangizo a Davide ouzilidwa akuti: “Umutulile Yehova Nkhawa Zako.”

Tingatsatile bwanji malangizo amenewa?

55:22

Davide apemphela
  1. Mukakumana ndi vuto kapena mukakhala ndi nkhawa, pemphelani kwa Yehova mocokela pansi pamtima

  2. Pezani thandizo kucokela m’Mau a Yehova ndi gulu lake

  3. Citani zimene mungakwanitse kuti muthetse vuto limenelo mogwilizana ndi mfundo za m’Baibulo

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani