LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb17 March tsa. 1
  • Maulaliki a Citsanzo

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Maulaliki a Citsanzo
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano —2017
  • Tumitu
  • Nkhani Zofanana
  • NSANJA YA MLONDA
  • KODI UFUMU WA MULUNGU N’CIANI?
  • Lemba: Dan. 2:44; Yes. 9:6
  • CIITANO CA KU CIKUMBUTSO
  • KONZANI ULALIKI WANU
  • Maulaliki Acitsanzo
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Msonkhano (2016)
  • Maulaliki a Citsanzo
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano —2017
  • Maulaliki a Citsanzo
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Msonkhano (2016)
  • Maulaliki a Citsanzo
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano —2017
Onaninso Zina
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano —2017
mwb17 March tsa. 1
Amboni za Yehova ku Albania agaŵila kapepa ka Ciitano ca ku Cikumbutso

Aitanila anthu ku Mgonelo wa Ambuye ku Albania

Maulaliki a Citsanzo

NSANJA YA MLONDA

Nsanja ya Mlonda ya Na. 2 2017 | Kodi Mudzalandila Mphatso Yaikulu Koposa?

Funso: M’kuona kwanu, muganiza mphatso yopambana zonse imene Mulungu anatipatsa ni iti?

Lemba: Yoh. 3:16

Cogaŵila: Magaziniyi ifotokoza cifukwa cake Mulungu anatuma Yesu kudzatifela, na mmene tingaonetsele kuyamikila mphatso imeneyo.

KODI UFUMU WA MULUNGU N’CIANI?

Kodi Ufumu wa Mulungu N’ciani?

Funso: [Muonetseni kapepa kauthenga.] Mungayankhe bwanji funso iyi? Kodi ufumu wa Mulungu ni cinacake cimene cili mumtima mwanu? mau okuluŵika? kapena boma lakumwamba?

Lemba: Dan. 2:44; Yes. 9:6

Cogaŵila: Kapepa aka kaonetsa mmene Ufumu wa Mulungu ungakupindulitsileni.

CIITANO CA KU CIKUMBUTSO

Kapepa ka Ciitano ca ku Cikumbutso ka 2017

Kugaŵila Kapepa ka Ciitano: Tiitanila anthu ku cocitika cofunika kwambili. [Mpatseni ciitano.] Pa 11 April, anthu mamiliyoni padziko lonse adzasonkhana kuti akumbukile imfa ya Yesu, na kumvetsela nkhani ya Baibo kwaulele. Nkhaniyo idzaonetsa mmene tingapindulile na imfa ya Yesu. Kapepa ka ciitano aka kaonetsa nthawi na malo kumene kudzacitikila mwambo umenewu kuno kwathu. Tidzakondwela ngati mungabwele.

KONZANI ULALIKI WANU

Funso:

Lemba:

Cogaŵila:

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani