LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb18 September tsa. 2
  • Yesu Acita Cozizwitsa Cake Coyamba

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Yesu Acita Cozizwitsa Cake Coyamba
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2018
  • Nkhani Zofanana
  • “Mukhale Oyela”
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2019
  • Yehova Analenga Zamoyo pa Dziko Lapansi
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2020
  • “Macimo Ako Akhululukidwa”
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2018
  • Kodi Yesu ni Munthu Wotani?
    Kondwelani Na Moyo Kwamuyaya!—Maphunzilo a Baibo Okambilana Komanso Zocita
Onaninso Zina
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2018
mwb18 September tsa. 2

CUMA COPEZEKA M’MAU A MULUNGU | YOHANE 1-2

Yesu Acita Cozizwitsa Cake Coyamba

2:1-11

Cozizwitsa coyamba ca Yesu citithandiza kudziŵa bwino umunthu wake. Kodi nkhani ya m’Baibo imeneyi ionetsa bwanji kuti?

  • Yesu sanali kukonda zosangalatsa mopambanitsa komanso anali kupatula nthawi kuti asangalale na anzake

  • Yesu anali woganizila ena

  • Yesu anali wopatsa

Yesu alamula kuti anthu athile madzi m’mbiya, woyang’anila phwando la cikwati alaŵa vinyo, ndiyeno ayamikila mkwati cifukwa ca vinyo wabwino.
    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani