LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb22 January tsa. 6
  • Pitilizani Kuonetsa Cikondi Cosasintha

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Pitilizani Kuonetsa Cikondi Cosasintha
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2022
  • Nkhani Zofanana
  • Pitilizani Kuonetsana Cikondi Cosasintha
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2021
  • Rute na Naomi
    Maphunzilo Amene Tingatengemo m’Baibo
  • Rute Ndi Naomi
    Buku Langa La Nkhani Za M’baibo
  • Mungamutumikile Yehova Ngakhale Kuti Makolo anu Sanapeleke Citsanzo Cabwino
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2023
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2022
mwb22 January tsa. 6

CUMA COPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

Pitilizani Kuonetsa Cikondi Cosasintha

[Onetsani vidiyo yakuti Mfundo Zokhudza Buku la Rute.]

Naomi anacondelela Olipa na Rute kuti abwelele ku Mowabu (Rute 1:8-13; w16.02 10 ¶5)

Rute anakana kusiya Naomi komanso Yehova. (Rute 1:16, 17; w16.02 10 ¶6)

Zithunzi: 1. Mayi na mwana wake wamkazi akuceza na banja lina pa vidiyo. 2. Banjalo labweletsela mayiyo na mwana wake cakudya cokonzedwa kale na basiketi ya zakudya zina.

Munthu amaonetsa cikondi cosasintha cifukwa ca mtima wodzipeleka, kukhulupilika, na cikondi cozama. Yehova amaonetsa cikondi cosasintha kwa atumiki ake okhulupilika. (Sal. 63:3) Ifenso tiyenela kuonetsa cikondi cosasintha kwa ena.—Miy. 21:21.

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani