LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb22 May tsa. 5
  • “Cikondi . . . Cimayembekezela Zinthu Zonse”

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • “Cikondi . . . Cimayembekezela Zinthu Zonse”
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2022
  • Nkhani Zofanana
  • “Cikondi . . . Sicidzikuza”
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2022
  • Ciyembekezo Cathu N’cosagwilitsa Mwala
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2023
  • Zifukwa Zokhalila na Ciyembekezo mu 2023—Kodi Baibo Ikutipo Ciyani?
    Nkhani Zina
  • Tengelani Citsanzo ca Atumiki Okhulupilika a Yehova
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2016
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2022
mwb22 May tsa. 5

UMOYO WATHU WACIKHRISTU

“Cikondi . . . Cimayembekezela Zinthu Zonse”

Cifukwa tili na cikondi copanda dyela, timawafunila zabwino abale athu. (1 Akor. 13:4, 7) Mwacitsanzo, ngati m’bale wacita chimo ndipo wapatsidwa cilango, timakhala na ciyembekezo cakuti adzacitapo kanthu na kusintha. Timaleza nawo mtima aja ofooka m’cikhulupililo, ndipo timayesetsa kuwathandiza. (Aroma 15:1) Ngati wina wasankha kucoka mumpingo, sitileka kuyembekezela kuti tsiku lina adzabwelela.—Luka 15:17, 18.

ONELELANI VIDIYO YAKUTI KUMBUKILANI MMENE CIKONDI CILILI—CIMAYEMBEKEZELA ZINTHU ZONSE, NDIYENO YANKHANI MAFUNSO OTSATILAWA:

  • Kodi Abineri anasintha n’kukhala wokhulupilika kwa ndani? Fotokozani

  • Kodi Davide analilandila bwanji pempho la Abineri? Nanga Yowabu analilandila motani?

  • N’cifukwa ciyani tiyenela kuwafunila zabwino abale athu?

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani