LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb23 September tsa. 10
  • Umoyo Ukafika Poti Simungathenso Kupilila

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Umoyo Ukafika Poti Simungathenso Kupilila
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2023
  • Nkhani Zofanana
  • Kodi Mukumbukila?
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2020
  • “Yembekezela Yehova”
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2022
  • Kodi Yobu Anali Ndani?
    Maphunzilo Amene Tingatengemo m’Baibo
  • Yobu Anapewa Maganizo Olakwika
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Msonkhano (2016)
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2023
mwb23 September tsa. 10

CUMA COPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

Umoyo Ukafika Poti Simungathenso Kupilila

Pa nthawi ya masautso, Yobu anayelekezela umoyo wake na nchito yokakamiza (Yobu 7:1; w06 3/15 14 ¶10)

Mavuto amene anakumana nawo anam’pangitsa kukamba zonse za mumtima mwake (Yobu 7:11)

Anafika ngakhale pokamba kuti anali kulakalaka kufa (Yobu 7:16; w20.12 16 ¶1)

M’bale wacinyamata ali na bwenzi lake lacikulile kunyumba kwake, ndipo akulifotokozela mmene akumvela.

Ngati inunso muona kuti umoyo wafika poti simungathenso kupilila, mwa pemphelo m’khuthulileni Yehova za mumtima mwanu. Komanso uzankoni mnzanu wokhwima maganizo mmene mumvela. Kucita zimenezi kungakuthandizeni kuyamba kumvako bwino.—g 1/12 16-17.

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani