LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb23 November tsa. 15
  • Cifukwa Cake Kuonelela Zamalisece N’koipa

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Cifukwa Cake Kuonelela Zamalisece N’koipa
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2023
  • Nkhani Zofanana
  • Kodi Zamalisece Zilibe Vuto?
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova—2013
  • Zisankho Zimene Zimaonetsa Kuti Timadalila Yehova
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2023
  • Mmene Tingadzitetezele ku Msampha wa Satana
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2019
  • Ngati Mnzanu wa mu Ukwati Amaonelela Zamalisece
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2023
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2023
mwb23 November tsa. 15

UMOYO WATHU WACIKHRISTU

Cifukwa Cake Kuonelela Zamalisece N’koipa

Masiku ano, zamalisece zili paliponse ndipo n’zosavuta kupeza. Anthu ambili, ngakhale opembedza amaona kuti kutamba zamalisece kulibe vuto.

Zithunzi: Zithunzi za muvidiyo yakuti “Kodi Kuonelela Zamalisece N’kucimwila Mulungu?” 1. Amuna aŵili na mkazi mmodzi akuseŵenzetsa mafoni awo poyembekeza basi. Amuna aŵiliwo akuonelela zinthu zolembedwa “XXX.” 2. Pambuyo pake, mwamuna mmodzi na mkazi wake akuwelenga nkhani yakuti “Kodi Baibulo Limaletsa Kuonera Zolaula?” pa jw.org.

TAMBANI VIDIYO YAKUTI KODI KUONELELA ZAMALISECE N’KUCIMWILA MULUNGU? KENAKO YANKHANI FUNSO ILI:

Kodi malemba awa amatithandiza bwanji kumvetsa mmene Mulungu amaonela zamaliseche?

  • 1 Akor. 6:​9, 10

  • Mat. 5:28

  • Akol. 3:5

  • Yak. 1:​14, 15

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani