LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • wp21 na. 1 tsa. 2
  • Mawu Oyamba

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Mawu Oyamba
  • Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yogawila)—2021
  • Nkhani Zofanana
  • Kodi Mulungu Amamva Mapemphelo Athu?
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yogawila)—2021
  • Yandikilani kwa Mulungu Kupitila M’pemphelo
    Zimene Baibo Imaphunzitsa M’ceni-ceni
  • Mmene Yehova Amayankhila Mapemphelo Athu
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2023
  • Gao 11
    Mvetselani kwa Mulungu
Onaninso Zina
Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yogawila)—2021
wp21 na. 1 tsa. 2

Mawu Oyamba

Kodi nthawi zina mumaona monga Mulungu sanayankhe mapemphelo anu? Ngati n’conco, dziŵani kuti si imwe mwekha. Ambili apemphelapo kwa Mulungu kuti awathandize pa vuto lawo, koma vutolo silinathe. Nkhani za m’magazini ino zifotokoza cifukwa cake tiyenela kukhulupilila kuti Mulungu amamvetsela mapemphelo athu, cifukwa cake sayankha mapemphelo ena, komanso mmene mungapemphelele kuti azimvetsela mapemphelo anu.

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani