LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • wp21 na. 1 tsa. 16
  • Kodi Mulungu Amamva Mapemphelo Anu?

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Kodi Mulungu Amamva Mapemphelo Anu?
  • Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yogawila)—2021
  • Tumitu
  • Nkhani Zofanana
  • ZIMENE BAIBO IMAKAMBA
  • Kodi Mulungu Amamva Mapemphelo Athu?
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yogawila)—2021
  • N’cifukwa Ciani Mulungu Amatilimbikitsa Kupemphela?
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova—2015
  • Mwayi Wa Pemphelo
    Zimene Baibulo Ingatiphunzitse
  • Kodi Pali Amene Akumvetsela?
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova—2015
Onaninso Zina
Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yogawila)—2021
wp21 na. 1 tsa. 16

Kodi Mulungu Amamva Mapemphelo Anu?

Mukamapemphela, kodi muganiza kuti Mulungu amamvadi mapemphelo anu?

ZIMENE BAIBO IMAKAMBA

Mayi akuŵelenga Baibo.
  • Mulungu amamvetsela. Baibo imatitsimikizila kuti “Yehova ali pafupi ndi onse oitanila pa iye. Iye ali pafupi ndi onse amene amamuitana m’coonadi. . . . Adzamva kufuula kwawo kopempha thandizo.”—Salimo 145:18, 19.

  • Mulungu amafuna kuti muzipemphela kwa iye. Baibo imati: “Pa ciliconse, mwa pemphelo ndi pembedzelo, pamodzi ndi ciyamiko, zopempha zanu zidziŵike kwa Mulungu.” —Afilipi 4:6.

  • Mulungu amasamala kwambili za imwe. Mulungu amadziŵa bwino kwambili mavuto athu na nkhawa zathu, ndipo amafuna kutithandiza. Baibo imati: “Citani zimenezi pamene mukumutulila nkhawa zanu zonse, pakuti amakudelani nkhawa.”—1 Petulo 5:7.

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani