LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb18 July tsa. 2
  • Tizipimila Ena Mowolowa Manja

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Tizipimila Ena Mowolowa Manja
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2018
  • Nkhani Zofanana
  • Opatsa Mowoloŵa Manja Amakhala Acimwemwe
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2018
  • Kuti Banja Likhale Lacimwemwe: Muziwelenga Mau a Mulungu
    Mfundo Zothandiza m’Banja
  • Njila Yoonetsela Kuyamikila
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2020
  • “Tsopano Uona Zimene Ndicite kwa Farao”
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2020
Onaninso Zina
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2018
mwb18 July tsa. 2

CUMA COPEZEKA M’MAU A MULUNGU | LUKA 6-7

Tizipimila Ena Mowolowa Manja

6:38

Munthu wowolowa manja amapeleka mokondwela nthawi yake, mphamvu zake, na zinthu zake kuti athandize ena na kuwalimbikitsa.

  • Munthu wa m’nthawi ya Baibo wanyamula mbewu pa covala cake

    Mau a Cigiriki amene anawamasulila kuti “khalani opatsa” atanthauza kucita cinthu mosalekeza

  • Ngati tikhala opatsa, ena adzatikhuthulila m’matumba athu “muyezo wabwino, wotsendeleka, wokhuchumuka ndi wosefukila.” Mau amenewa angatanthauze cizoloŵezi ca ogulitsa malonda amene amaikapo mbasela pa zinthu zimene munthu wagula

M’bale wacicepele athandiza m’bale wacikulile kunyamula zinthu zimene wagula.

Ndandalikani zocitika pamene imwe mungaseŵenzetse malangizo amenewa.

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani